Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w10 7/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2010
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:
Nsanja ya Olonda—2010
w10 7/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

July 15, 2010

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

August 30, 2010–September 5, 2010

Kodi pa Tsiku la Yehova Padzachitika Zotani?

TSAMBA 3

NYIMBO ZOIMBA: 30, 40

September 6-12, 2010

“Lingalirani za Mtundu wa Munthu Amene Muyenera Kukhala”

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 48, 29

September 13-19, 2010

Muzigwira Nawo Mokwanira Ntchito Yokolola Mwauzimu

TSAMBA 16

NYIMBO ZOIMBA: 45, 28

September 20-26, 2010

“Mzimu Umafufuza . . . Zinthu Zozama za Mulungu”

TSAMBA 20

NYIMBO ZOIMBA: 38, 20

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA 1, 2 MASAMBA 3-11

M’kalata yake yachiwiri, mtumwi Petulo anasonyeza kuti ankadera nkhawa kwambiri Akhristu a m’masiku otsiriza. Nkhani ziwiri zimenezi zitithandiza kuti tizikumbukira tsiku la Yehova nthawi zonse. Tikambirana zinthu zimene tiyenera kupewa ndiponso zimene tiyenera kuchita pokonzekera tsiku lalikulu la Yehova.

NKHANI YOPHUNZIRA 3 MASAMBA 16-20

Tikukhala m’nthawi imene ntchito yaikulu yokolola mwauzimu ikuchitika. Kodi tiyenera kukhala ndi makhalidwe ati, kuti tizigwira nawo mokwanira ntchito yokololayi? Ngakhale pamene zinthu pa moyo wathu sizili bwino, kodi tingatani kuti tizigwirabe nawo mokwanira ntchito yolalikira? Nkhaniyi ikuyankha mafunso amenewa.

NKHANI YOPHUNZIRA 4 MASAMBA 20-24

Nkhaniyi ikufotokoza zimene aliyense payekha angachite kuti apindule ndi zimene mzimu wa Mulungu ukuchita potithandiza kumvetsa Mawu ake.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:

“Usaope Ndidzakuthandiza” 12

Thandizani Ana Anu Kuti Azikonda Kuwerenga ndi Kuphunzira 25

‘Pitiriza Kudzipereka pa Kuphunzitsa’ 29

Kukhala Tcheru Kumakhala ndi Zotsatira Zabwino 32

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena