Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w10 8/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2010
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:
Nsanja ya Olonda—2010
w10 8/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

August 15, 2010

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

September 27, 2010–October 3, 2010

Kodi Yesu Amasonyeza Bwanji Chilungamo cha Mulungu?

TSAMBA 8

NYIMBO ZOIMBA: 46, 49

October 4-10, 2010

Mmene Dipo Limatipulumutsira

TSAMBA 12

NYIMBO ZOIMBA: 31, 30

October 11-17, 2010

Muzitsatira Lamulo la Kukoma Mtima Polankhula

TSAMBA 21

NYIMBO ZOIMBA: 35, 50

October 18-24, 2010

Kodi Ndani Angathandize Anthu Ovutika?

TSAMBA 28

NYIMBO ZOIMBA: 38, 23

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA 1, 2 MASAMBA 8-16

M’nkhani ino tiphunzira mmene Satana anatsutsira Mulungu. Tiona mmene Yesu anasonyezera kuti Yehova ndi woyenera kulamulira. Tionanso zimene Yesu anafunika kuchita kuti apereke nsembe ya dipo komanso mmene dipolo lingakupulumutsireni.

NKHANI YOPHUNZIRA 3 MASAMBA 21-25

M’nkhaniyi tiphunzira tanthauzo la kukoma mtima ndiponso mmene kumakhudzira kalankhulidwe kathu. Tionanso zimene tingachite kuti tsiku lililonse tizilankhula mokoma mtima.

NKHANI YOPHUNZIRA 4 MASAMBA 28-32

Salmo 72 limasonyeza bwino zimene zidzachitike mu Ulamulira wa zaka 1,000 wa Mwana wa Mulungu, Yesu Khristu. Mudzalimbikitsidwa kuphunzira nkhani imeneyi ndiponso kuganizira mmene Yehova adzagwiritsire ntchito Solomo Wamkulu populumutsa anthu osowa thandizo.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:

Pewani Kuyendera Maganizo a Anthu Ena 3

Mafunso Ochokera kwa Owerenga 6

Mukuitanidwa! 17

Kodi Mukukumbukira? 20

N’chifukwa Chiyani Muyenera Kusunga Nthawi? 25

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena