Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w10 10/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2010
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:
Nsanja ya Olonda—2010
w10 10/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

October 15, 2010

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

November 29, 2010–December 5, 2010

“Ndani Akudziwa Maganizo a Yehova?”

TSAMBA 3

NYIMBO ZOIMBA: 11, 51

December 6-12, 2010

Pitirizani Kufunafuna Choyamba “Chilungamo Chake”

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 40, 22

December 13-19, 2010

Kodi Mumakhala Patsogolo Posonyeza Ulemu kwa Akhristu Anzanu?

TSAMBA 16

NYIMBO ZOIMBA: 31, 9

December 20-26, 2010

Kodi Mumathandiza Kuti Misonkhano Yachikhristu Ikhale Yolimbikitsa?

TSAMBA 20

NYIMBO ZOIMBA: 20, 34

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA 1, 2 MASAMBA 3-11

Nkhanizi zitithandiza kuona zimene tingachite kuti tikhale pa ubwenzi wabwino ndi Yehova mwa kuphunzira za Yesu. Zikufotokozanso tanthauzo la chilungamo cha Mulungu, chifukwa chake tiyenera kuchifunafuna choyamba, ndiponso chifukwa chake sitiyenera kuweruza Yehova pogwiritsa ntchito mfundo zathu.

NKHANI YOPHUNZIRA 3 MASAMBA 16-20

Kodi chimafunika n’chiyani kuti tizilemekeza Akhristu anzathu? N’chifukwa chiyani tiyenera kuwalemekeza? Kodi tingatani kuti tikhale patsogolo pa nkhani yosonyeza ulemu? Amenewa ndi ena mwa mafunso amene tikambirane mu nkhaniyi.

NKHANI YOPHUNZIRA 4 MASAMBA 20-25

Nkhaniyi ikufotokoza zimene otsogolera pa misonkhano yachikhristu komanso ena onse angachite kuti misonkhano yathu izikhala yolimbikitsa. Ikufotokozanso zinthu zina zimene zasintha m’magazini yophunzira.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:

Kodi Yehova Amaona Bwanji Kupereka Zifukwa Pofuna Kudzikhululukira 12

Thandizani Ana Kulidziwa Bwino Gulu la Yehova 25

Ndimayesetsa Kukhala ndi Zochita Zambiri M’gulu la Yehova 29

“Kabuku Kamene Kamandithandiza Kuwafika Anthu pa Mtima” 32

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena