Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w10 11/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2010
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:
Nsanja ya Olonda—2010
w10 11/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

November 15, 2010

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

December 27, 2010–January 2, 2011

Achinyamata, Muzitsogoleredwa ndi Mawu a Mulungu

TSAMBA 3

NYIMBO ZOIMBA: 37, 22

January 3-9, 2011

Achinyamata, Pewani Kutengera Zochita Za Anzanu

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 24, 52

January 10-16, 2011

Achinyamata, Kodi Moyo Wanu Mudzaugwiritsa Ntchito Bwanji?

TSAMBA 12

NYIMBO ZOIMBA: 1, 11

January 17-23, 2011

Yehova Ndiye Ambuye Wathu Wamkulu Koposa

TSAMBA 24

NYIMBO ZOIMBA: 23, 51

January 24-30, 2011

Tidzayenda Mogwirizana ndi Mtima Wathu Wosagawanika

TSAMBA 28

NYIMBO ZOIMBA: 29, 45

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA 1-3 MASAMBA 3-16

Nkhani izi zakonzedwa kuti zithandize achinyamata. Nkhani yoyamba ikusonyeza zimene achinyamata angachite kuti azitsogoleredwa ndi malangizo opezeka m’Mawu a Mulungu, Baibulo. Nkhani yachiwiri ikusonyeza mmene angapewere kutengera zochita za anzawo. Nkhani yomaliza ikufotokoza zolinga zimene achinyamata angakhale nazo ndiponso zimene angazikwaniritsedi.

NKHANI ZOPHUNZIRA 4, 5 MASAMBA 24-32

M’nkhanizi tiphunzira zimene tingachite kuti tikhale kumbali ya ulamuliro wa Yehova Mulungu. Tiphunziranso zimene tingachite kuti tikhale ndi mtima wosagawanika. Tikambirana zinthu zimene zinachitika pa moyo wa Yobu yemwe anali wolungama. Nkhani zimenezi zitithandiza kukhala ndi mtima wosagawanika komanso kuona kuti Yehova ndi Ambuye wathu Wamkulu ngati mmene Yobu ndi atumiki ena a m’mbuyomu anachitira.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:

Yehova Amamva Kulira kwa Anthu Amtima Wachisoni 17

‘Aliyense Apereke Chopereka kwa Yehova’ 20

Mafunso Ochokera kwa Owerenga 22

Zabwino ‘Zimene Anachita Zapita Naye Limodzi’ 23

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena