Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w11 1/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2011
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:
Nsanja ya Olonda—2011
w11 1/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

January 15, 2011

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

February 28, 2011–March 6, 2011

‘Pezani Chitetezo M’dzina la Yehova’

TSAMBA 3

NYIMBO ZOIMBA: 49, 14

March 7-13, 2011

Muzilemekeza Ukwati Monga Mphatso Yochokera kwa Mulungu

TSAMBA 13

NYIMBO ZOIMBA: 36, 40

March 14-20, 2011

Muzigwiritsa Ntchito Mwanzeru Nthawi Imene Simuli pa Banja

TSAMBA 17

NYIMBO ZOIMBA: 26, 53

March 21-27, 2011

Mzimu Woyera Umatipatsa Mphamvu Yolimbana ndi Mayesero Ndiponso Zofooketsa

TSAMBA 22

NYIMBO ZOIMBA: 54, 17

March 28, 2011–April 3, 2011

Mzimu Woyera Umatipatsa Mphamvu Yolimbana ndi Vuto Lililonse

TSAMBA 26

NYIMBO ZOIMBA: 49, 17

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI YOPHUNZIRA 1 MASAMBA 3-7

Kodi tingapeze kuti chitetezo m’masiku ovuta ano? Mawu a Mulungu amanena kuti tikhoza kupeza chitetezo m’dzina la Yehova. M’nkhaniyi tikambirana mmene tingapezere chitetezo masiku ano komanso “tsiku lalikulu la Yehova” likadzafika. Nkhaniyi ikufotokoza bwino lemba la chaka cha 2011.

NKHANI ZOPHUNZIRA 2, 3 MASAMBA 13-21

Ukwati ndiponso kukhala wosakwatira kapena wosakwatiwa ndi mphatso zochokera kwa Mulungu. Mphatso zonsezi ndi zabwino. Kaya tili m’banja kapena ayi, nkhanizi zifotokoza zifukwa zotithandiza kuyamikira mphatsozi ndiponso mmene tingasonyezere kuyamikira.

NKHANI ZOPHUNZIRA 4, 5 MASAMBA 22-30

Timafuna thandizo la Yehova kuti tikwaniritse kudzipereka kwathu kwa iye. Nkhanizi zifotokoza mmene mzimu woyera umatithandizira kulimbana ndi mayesero ndiponso zinthu zofooketsa, kupirira chizunzo ndi mavuto komanso kupewa kumangotengera zochita za  anzathu.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:

7 Dzina la Mulungu M’chigwa cha ku Switzerland

9 Ndimayamikira Kutumikira Yehova, Ngakhale pa Nthawi Zovuta

31 Muziganizira Zimene Yehova Wakuchitirani Kale

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

© Stähli Rolf A/​age fotostock

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena