Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w11 3/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2011
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:
Nsanja ya Olonda—2011
w11 3/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

March 15, 2011

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

May 2-8, 2011

Landirani Mzimu wa Mulungu Osati wa Dziko

TSAMBA 8

NYIMBO ZOIMBA: 23, 38

May 9-15, 2011

Muzidalira Yehova Pamene Mapeto Akuyandikira

TSAMBA 12

NYIMBO ZOIMBA: 43, 48

May 16-22, 2011

Khalani Okonzeka

TSAMBA 24

NYIMBO ZOIMBA: 54, 24

May 23-29, 2011

Khalanibe Tcheru Ngati Yeremiya

TSAMBA 28

NYIMBO ZOIMBA: 32, 43

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI YOPHUNZIRA 1 TSAMBA 8-12

Anthu ambiri amasonyeza mzimu wa dziko ndiye kodi n’zotheka kukhala osiyana nawo? Nkhaniyi itithandiza kuona mmene mzimu wa dziko ungayambire kutitsogolera. Tikambirananso zimene tikuphunzira kwa Yesu pa nkhani yolandira mzimu wa Mulungu.

NKHANI YOPHUNZIRA 2 TSAMBA 12-16

Kodi kudalira Yehova kumatanthauza chiyani? Nkhaniyi itithandiza kuona kuti kudalira Yehova sikumangotanthauza kukhulupirira malonjezo ake onena za dziko latsopano. Kumatanthauzanso kuvomereza ndi mtima wonse njira zake ndiponso mfundo zake, n’kumakana njira ndi mfundo za dzikoli.

NKHANI ZOPHUNZIRA 3, 4 TSAMBA 24-32

M’nkhanizi tidziwa zimene zinathandiza Nowa ndi banja lake, Mose ndiponso Yeremiya kukhalabe tcheru kuti akwaniritse ntchito zimene anapatsidwa. Onsewa adzaona kukwaniritsidwa kwa malonjezo a Mulungu. Onani zimene mungaphunzire kwa anthu amenewa komanso mtima umene anali nawo.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:

3 Musamadzinyenge ndi Maganizo Onama

6 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

17 Zinthu Zimene Mungakondwere Nazo

20 Musasiye Okhulupirira Anzanu

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena