Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w11 4/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2011
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2011
w11 4/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

April 15, 2011

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

May 30, 2011–June 5, 2011

Tiziona Kuti Kutumikira Yehova Ndi Chinthu Chofunika Kwambiri

TSAMBA 9

NYIMBO ZOIMBA: 43, 10

June 6-12, 2011

Zosankha Zanu Zizilemekeza Mulungu

TSAMBA 13

NYIMBO ZOIMBA: 2, 9

June 13-19, 2011

“Makhalidwe Amene Mzimu Woyera Umatulutsa” Amalemekeza Mulungu

TSAMBA 18

NYIMBO ZOIMBA: 25, 11

June 20-26, 2011

Kodi Mukulola Mzimu wa Mulungu Kukutsogolerani?

TSAMBA 23

NYIMBO ZOIMBA: 6, 48

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI YOPHUNZIRA 1 TSAMBA 9-13

M’dzikoli anthu ambiri sazindikira zinthu zofunika kwambiri, koma Akhristu sayenera kutero. Mkhristu ayenera kuona kulambira Yehova kukhala nkhani yofunika kwambiri. Nkhaniyi itithandiza kuona zinthu moyenera. Pogwiritsa ntchito Malemba, itithandizanso kudziwa mmene tiyenera kuonera maudindo athu achikhristu.

NKHANI YOPHUNZIRA 2 TSAMBA 13-17

Anthu ambiri amavutika kusankha zochita. Nkhaniyi itithandiza kudziwa chifukwa chake tiyenera kuphunzira kusankha zochita mwanzeru. Itchulanso mfundo zothandiza zimene tingatsatire kuti tizisankha zinthu zimene zimalemekeza Mulungu.

NKHANI ZOPHUNZIRA 3, 4 TSAMBA 18-27

Kodi “makhalidwe amene mzimu woyera umatulutsa” ndi ati? Kodi tingatani kuti tikhale nawo? N’chifukwa chiyani tiyenera kukhala nawo? Mukhoza kuyankha mafunso amenewa tikakambirana makhalidwe 9 amene mzimu woyera umatulutsa. Nkhanizi zili ndi mfundo zothandiza zimene anthu ambiri angapindule nazo.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

3 Kodi Mumaona Umboni Wakuti Mulungu Akutitsogolera?

6 Khalanibe Oona Mtima M’dziko la Anthu Osaona Mtima

28 Kodi Mukukumbukira?

29 Ndapeza Zinthu Zambiri Zabwino

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena