Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w11 5/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2011
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2011
w11 5/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

May 15, 2011

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

June 27, 2011–July 3, 2011

Mabanja Achikhristu Ayenera ‘Kukhalabe Maso’

TSAMBA 7

NYIMBO ZOIMBA: 11, 22

July 4-10, 2011

Mabanja Achikhristu Ayenera ‘Kukhala Okonzeka’

TSAMBA 11

NYIMBO ZOIMBA: 32, 18

July 11-17, 2011

Kodi Munthu Wofunika Kwambiri pa Moyo Wanu Ndi Ndani?

TSAMBA 16

NYIMBO ZOIMBA: 51, 49

July 18-24, 2011

‘Nzeru za Mulungu N’zozama’ Kwambiri

TSAMBA 21

NYIMBO ZOIMBA: 1, 43

July 25-31, 2011

Anthu Amene Amakhulupirira Yehova Amakhala Olimba Mtima

TSAMBA 28

NYIMBO ZOIMBA: 46, 23

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA 1, 2 TSAMBA 7-15

Nkhani yoyamba ikufotokoza udindo umene aliyense m’banja lachikhristu ali nawo kuti akhalebe maso mwauzimu. Nkhani yachiwiri ikufotokoza zinthu zofunika kwambiri kuti banja lonse lipite patsogolo mwauzimu. Zinthu zake ndizo kukhala ndi diso lolunjika pa chinthu chimodzi, kukhala ndi zolinga zauzimu ndiponso kuchita Kulambira kwa Pabanja nthawi zonse.

NKHANI YOPHUNZIRA 3 TSAMBA 16-20

Yehova ayenera kukhala wofunika kwambiri pa moyo wa atumiki ake. Nkhaniyi ikufotokoza zimene tingaphunzire kwa mkazi woyamba, Hava, munthu wokhulupirika, Yobu, ndiponso Yesu Khristu, yemwe ndi Mwana wangwiro wa Mulungu.

NKHANI YOPHUNZIRA 4 TSAMBA 21-25

Pa Aroma chaputala 11, mtumwi Paulo ananena za mtengo wa maolivi wophiphiritsa. Kodi mbali zosiyanasiyana za mtengo umenewu zimaimira chiyani? Pamene tikukambirana tanthauzo lake, tiphunzira zambiri zokhudza cholinga cha Yehova ndiponso tigoma ndi kuzama kwa nzeru zake.

NKHANI YOPHUNZIRA 5 TSAMBA 28-32

Nkhaniyi ikufotokoza Masalimo 3 ndi 4 amene Mfumu Davide analemba. Nyimbo zouziridwa ndi Mulungu zimenezi zimasonyeza kuti tikhoza kukhala olimba mtima ngati timapemphera kuti Yehova atithandize ndiponso ngati timamukhulupirira ndi mtima wonse. Izi ndi zimene Davide anachita pamene anakumana ndi mavuto monga kuukiridwa ndi mwana wake Abisalomu.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

3 Kodi Mumasangalala Kuwerenga Mawu a Mulungu?

6 “Woyang’anira Wabwino Ndiponso Mnzathu Wapamtima”

26 Tsatirani Khristu Yemwe Ndi Mtsogoleri Wabwino Kwambiri

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena