Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w11 11/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2011
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:
  • Cholinga cha Nkhani Zophunzira
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2011
w11 11/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

November 15, 2011

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA MILUNGU YA:

December 26, 2011–January 1, 2012

“Usadalire Luso Lako Lomvetsa Zinthu”

TSAMBA 6

NYIMBO ZOIMBA: 133, 23

January 2-8, 2012

Yendani Mogwirizana ndi Mzimu Kuti Mupeze Moyo ndi Mtendere

TSAMBA 10

NYIMBO ZOIMBA: 83, 120

January 9-15, 2012

Ndife “Osakhalitsa” M’dziko Loipali

TSAMBA 16

NYIMBO ZOIMBA: 40, 85

January 16-22, 2012

Thandizani Amuna Kukula Mwauzimu

TSAMBA 24

NYIMBO ZOIMBA: 123, 95

January 23-29, 2012

Thandizani Ena Kuti Ayenerere Maudindo

TSAMBA 28

NYIMBO ZOIMBA: 45, 10

Cholinga cha Nkhani Zophunzira

NKHANI YOPHUNZIRA 1 TSAMBA 6-10

Kodi mukugwiritsira ntchito bwino mwayi wa pemphero umene Mulungu watipatsa? Phunzirani mmene pemphero lingakuthandizireni mukamakumana ndi mavuto, posankha zinthu zofunika kwambiri, kapena mukamalimbana ndi mayesero.

NKHANI YOPHUNZIRA 2 TSAMBA 10-14

Mtumwi Paulo anauza Akhristu a ku Roma kuti aziika maganizo awo pa zinthu za mzimu n’cholinga choti apeze moyo ndi mtendere. Onani mmene mungapindulire ndi malangizo amene anawapatsa.

NKHANI YOPHUNZIRA 3 TSAMBA 16-20

Nkhaniyi ikusonyeza kuti anthu okhulupirika akale ankakhala monga anthu “osakhalitsa m’dzikolo.” Otsatira oyambirira a Yesu anachitanso chimodzimodzi. Nanga bwanji Akhristu masiku ano? M’nkhaniyi tiona tanthauzo la kukhala monga anthu osakhalitsa m’dziko loipali.

NKHANI ZOPHUNZIRA 4, 5 TSAMBA 24-32

Mu mpingo mukufunika amuna ambiri kuti azitsogolera pa zinthu zauzimu. Yesu anathandiza amuna ambiri kumva uthenga wabwino ndiponso kuyenerera maudindo ena. Tiyeni tione njira zimene iye ankagwiritsa ntchito n’cholinga choti nafenso tithandize anthu amene timakumana nawo mu utumiki. Tionanso mmene tingathandizire amuna obatizidwa kuti ayenerere maudindo m’gulu la Yehova.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

3 Yehu Anamenyera Nkhondo Kulambira Koyera

15 “Panopa Ndine Wolumala, Koma Sindidzakhala Chonchi Mpaka Kalekale”

21 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

22 Kodi Mumasangalala ndi “Mwayi Wopereka Nawo Mphatso Zachifundo”?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena