Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w12 2/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2012
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2012
w12 2/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

February 15, 2012

© 2012 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino n’ngwathu.

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA

APRIL 2-8, 2012

Tsanzirani Yesu pa Nkhani Yokhala Maso

TSAMBA 3 • NYIMBO: 108, 74

APRIL 9-15, 2012

‘Khalani Olimba Mtima Kwambiri Ndipo Muchite Zinthu Mwamphamvu’

TSAMBA 10 • NYIMBO: 101, 92

APRIL 16-22, 2012

Thandizani Mpingo Kukhalabe ndi Maganizo Abwino

TSAMBA 18 • NYIMBO: 20, 75

APRIL 23-29, 2012

N’zotheka Kukhala Osangalala M’banja Limene Wina Si Mboni

TSAMBA 26 • NYIMBO: 76, 56

CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA

NKHANI YOPHUNZIRA 1 TSAMBA 3-7

N’chifukwa chiyani Yesu analimbikitsa otsatira ake kukhalabe maso? Nkhaniyi ikusonyeza mmene Khristu anasonyezera kuti anali maso padziko lapansi. Tiona njira zitatu zimene anasonyezera zimenezi komanso mmene tingamutsanzirire.

NKHANI YOPHUNZIRA 2 TSAMBA 10-14

Kodi tingapindule chilichonse poona mmene atumiki a Yehova otchulidwa m’Baibulo anasonyezera kulimba mtima? Nkhani ino iyankha funso limeneli ndipo itithandiza kuti nafenso tizichita zinthu molimba mtima.

NKHANI YOPHUNZIRA 3 TSAMBA 18-22

Munthu aliyense amakhala ndi khalidwe linalake lapadera. Nkhani ino itithandiza kuona mmene tingathandizire mpingo kukhala ndi maganizo abwino.

NKHANI YOPHUNZIRA 4 TSAMBA 26-30

Ngati munthu wina m’banja si mboni, Mkhristu amakumana ndi mayesero. Nkhani ino ikufotokoza zimene Akhristu amene ali m’mabanja oterewa angachite kuti m’banja mwawo mukhale mtendere komanso kuti athandize enawo kuphunzira choonadi.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

8 Ankalalikira Mawu a Mulungu Molimba Mtima

15 Kaduka ndi Khalidwe Limene Lingawononge Maganizo Athu

23 Natani Anali Wokhulupirika Ndipo Ankalimbikitsa Kulambira Koona

31 Kale Lathu

PATSAMBA LOYAMBA: Pa malo okwerera sitima ku New Delhi, m’dziko laIndia. Tsiku lililonse pamabwera masitima oposa 300. Abale amalalikira kwa anthu amene amabwera kudzagwira ntchito ndiponso kwa anthu apaulendo ochokera m’madera osiyanasiyana m’dzikoli

INDIA

KULI ANTHU OKWANA

1,224,614,000

KULI OFALITSA OKWANA

33,182

OFALITSA AWONJEZEKA NDI

5 peresenti

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena