Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w12 5/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2012
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2012
w12 5/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

May 15, 2012

© 2012 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino n’ngwathu.

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA

JULY 2-8, 2012

Muziyamikira Mphatso ya Ukwati Yochokera kwa Mulungu

TSAMBA 3 • NYIMBO: 87, 75

JULY 9-15, 2012

Musataye Mtima Ngati Banja Lanu Silikuyenda Bwino

TSAMBA 8 • NYIMBO: 36, 69

JULY 16-22, 2012

Khulupirirani Yehova, Mulungu wa “Nthawi ndi Nyengo”

TSAMBA 17 • NYIMBO: 116, 135

JULY 23-29, 2012

Kodi Mukuonetsa Ulemerero wa Yehova?

TSAMBA 23 • NYIMBO: 93, 89

CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA

NKHANI ZOPHUNZIRA 1, 2 TSAMBA 3-12

Nkhanizi zikusonyeza kuti kutsatira malangizo a Yehova pa nkhani ya ukwati n’kofunika kwambiri. Zitithandizanso kuyamikira kwambiri mphatso ya ukwati imene Mulungu wapereka. Zikufotokozanso kuti ngati banja lathu silikuyenda bwino sitiyenera kutaya mtima. Komanso zikufotokoza mmene kutsatira malangizo a m’Malemba kungatithandizire kuti tikhale ndi banja losangalala.

NKHANI YOPHUNZIRA 3 TSAMBA 17-21

Nkhaniyi ikufotokoza kuti Yehova amachita zinthu pa nthawi yake. Itithandiza kukhulupirira kwambiri Mulungu komanso Mawu ake, Baibulo. Itilimbikitsanso kugwiritsa ntchito mwanzeru nthawi yathu pamene tikuyembekezera mosakayikira kuti Yehova atipulumutsa.

NKHANI YOPHUNZIRA 4 TSAMBA 23-27

Anthufe ndife opanda ungwiro koma timakonda Mulungu. Komanso timafunitsitsa kuonetsa ulemerero wa Yehova. Nkhaniyi ikufotokoza mmene tingachitire zimenezi. Ikusonyezanso zimene tiyenera kuchita kuti tizitsanzira Mulungu ndiponso kumusangalatsa. (Aef. 5:1) Ikufotokozanso mmene tingapitirizire kuonetsa ulemerero wake.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

13 Ndinkakonda kucheza ndi Achikulire anzeru

22 Mafunso ochokera kwa Owerenga

28 “Samalani ndi chofufumitsa cha Afarisi”

31 Kale lathu

PATSAMBA LOYAMBA: Banja lomwe likuchita upainiya likulalikira kwa dalaivala pamalo oimika magalimoto akuluakulu mumzinda wa Toulouse ku France. Magalimoto akuluakulu oposa 1,800, ochokera mayiko osiyanasiyana a ku Ulaya, amadutsa mumzindawu tsiku lililonse.

FRANCE

KULI ANTHU OKWANA

63,787,000

KULI OFALITSA OKWANA

122,433

M’ZAKA 5 ZAPITAZI, APAINIYA AWONJEZEKA NDI:

119 Peresenti

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena