Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w12 9/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2012
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IYI
Nsanja ya Olonda—2012
w12 9/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

September 15, 2012

© 2012 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino ndi wathu.

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA

OCTOBER 22-28, 2012

Kodi Dzikoli Lidzatha Bwanji?

TSAMBA 3 • NYIMBO: 133, 132

OCTOBER 29, 2012–NOVEMBER 4, 2012

Mtendere Udzayamba mu Ulamuliro wa Zaka 1,000

TSAMBA 8 • NYIMBO: 55, 134

NOVEMBER 5-11, 2012

Tsanzirani Kuleza Mtima kwa Yehova ndi Yesu

TSAMBA 18 • NYIMBO: 35, 90

NOVEMBER 12-18, 2012

“Simukudziwa Tsiku Kapena Ola Lake”

TSAMBA 23 • NYIMBO: 43, 92

NOVEMBER 19-25, 2012

Yehova Amasonkhanitsa Anthu Ake Osangalala

TSAMBA 28 • NYIMBO: 119, 118

CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA

NKHANI ZOPHUNZIRA 1, 2 TSAMBA 3-12

Pali zinthu zikuluzikulu zimene zichitike posachedwapa. Nkhanizi zikufotokoza zinthu 10 zimene zichitike. Zinthu zisanu ndi zokhudza kuwononga dziko la Satanali ndipo zinazo ndi zokhudza kukhazikitsa dziko latsopano.

NKHANI YOPHUNZIRA 3 TSAMBA 18-22

Tonsefe timayembekezera nthawi imene zinthu zoipa zidzathe ndipo dzikoli lidzakhala Paradaiso. Kaya mwakhala mukuyembekezera kwa miyezi yochepa kapena zaka zambiri, kuleza mtima n’kofunika. Nkhaniyi ikufotokoza zimene zingatithandize kukhala oleza mtima kwambiri.

NKHANI YOPHUNZIRA 4 TSAMBA 23-27

Anthu onse a Mulungu akufuna kuti dziko loipali lithe basi. Nkhaniyi ikusonyeza kuti kusadziwa tsiku kapena ola la mapeto kuli ndi ubwino wake.

NKHANI YOPHUNZIRA 5 TSAMBA 28-32

Kuyambira kale, misonkhano ikuluikulu yakhala yofunika kwambiri kwa anthu a Mulungu. Nkhaniyi ikufotokoza misonkhano yosaiwalika yotchulidwa m’Baibulo ndiponso ya masiku ano. Ikufotokozanso ubwino wa kupezeka pa misonkhanoyi.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IYI

13 Sukulu Zophunzitsa Atumiki a Mulungu Zimasonyeza Kuti Yehova Amatikonda

PATSAMBA LOYAMBA: Abale ku Philippines amayesetsa kulalikira kwa anthu onse. Apa akulalikira kwa munthu yemwe ali pa njinga yokhala ndi kangolo ndipo ali kumpoto kwa chilumba cha Luzon

PHILIPPINES

KULI OFALITSA

177,635

APAINIYA OKHAZIKIKA

29,699

OBATIZIDWA MU 2011

8,586

AMAMASULIRA MABUKU M’ZINENERO

21

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena