Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w12 10/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2012
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2012
w12 10/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

October 15, 2012

© 2012 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino n’ngwathu.

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA

NOVEMBER 26, 2012–DECEMBER 2, 2012

Limbani Mtima Pokumana ndi Mavuto

TSAMBA 7 • NYIMBO: 81, 33

DECEMBER 3-9, 2012

Kodi Mumaonetsa Mzimu Wotani?

TSAMBA 12 • NYIMBO: 122, 124

DECEMBER 10-16, 2012

Mverani Mulungu Kuti Mupindule ndi Malumbiro Ake

TSAMBA 22 • NYIMBO: 129, 95

DECEMBER 17-23, 2012

Mukati Inde Akhaledi Inde

TSAMBA 27 • NYIMBO: 63, 125

CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA

NKHANI YOPHUNZIRA 1 TSAMBA 7-11

Masiku ano, mavuto ndi osachita kunena. Nkhaniyi itithandiza kuona zimene tikuphunzira kwa anthu akale ndiponso a masiku ano amene analimba mtima pokumana ndi mavuto aakulu. Ikufotokozanso zimene zingatithandize kukhala olimba mtima kwambiri ndiponso osangalala zivute zitani.

NKHANI YOPHUNZIRA 2 TSAMBA 12-16

Masiku ano, anthu salimbikitsana, m’malomwake amangokhumudwitsana. M’nkhani ino tiona zinthu zosokoneza mtendere mu mpingo zimene tiyenera kupewa. Tikambirananso zimene tingachite kuti tizigwirizana ndi anzathu.

NKHANI YOPHUNZIRA 3, 4 TSAMBA 22-31

Nkhani yoyamba ikusonyeza kuti Mulungu walumbira kuti akwaniritsa malonjezo ake. Kuti tidzapindule ndi malonjezowa, tiyenera kumvera Mulungu komanso kuchita zimene talonjeza. Nkhani yachiwiri ikufotokoza za anthu amene anachitadi zimene analonjeza. Ikulimbikitsa Akhristu onse obatizidwa kuti akwaniritse “Inde” wawo wofunika kwambiri.—Mat. 5:37.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

3 Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Brazil

17 Ubwenzi wa Zaka 60, Koma Akuti N’chiyambi Chabe

32 Mawu Olimbikitsa a “Ana Aang’ono”

PATSAMBA LOYAMBA: Banja limene likuchita upainiya, likulalikira kumbali ya mzinda kumene kumadutsa anthu ambiri. Likugwiritsa ntchito shelefu ya matayala

DERA LA TIMES SQUARE KU MANHATTAN, KU NEW YORK CITY

APAINIYA

600

AMALALIKIRA KU MANHATTAN M’MADERA

12

KULI MIPINGO

55

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena