Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w12 11/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2012
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2012
w12 11/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

November 15, 2012

© 2012 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino ndi wathu.

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA

DECEMBER 24-30, 2012

“Ndiphunzitseni Kuchita Chifuniro Chanu”

TSAMBA 3 • NYIMBO: 69, 120

DECEMBER 31, 2012–JANUARY 6, 2013

Yesu Anatipatsa Chitsanzo cha Kudzichepetsa

TSAMBA 10 • NYIMBO: 84, 82

JANUARY 7-13, 2013

Yesetsani Kukhala Ngati Wamng’ono

TSAMBA 15 • NYIMBO: 26, 68

JANUARY 14-20, 2013

Yehova Ndi Wofunitsitsa Kukukhululukirani

TSAMBA 21 • NYIMBO: 67, 91

JANUARY 21-27, 2013

Muzikhululukirana ndi Mtima Wonse

TSAMBA 26 • NYIMBO: 77, 118

CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA

NKHANI YOPHUNZIRA 1 TSAMBA 3-7

Mfumu Davide inkalemekeza kwambiri dzina la Yehova ndiponso cholinga chake. Nkhaniyi ikusonyeza kuti Davide ankalemekezanso mfundo za m’Chilamulo cha Mulungu ndipo ankapemphera kuti Mulungu amuphunzitse kuchita chifuniro chake. Nkhaniyi itithandizanso kuona kuti nthawi zonse tiyenera kuyesetsa kuona zinthu mmene Yehova amazionera.

NKHANI ZOPHUNZIRA 2, 3 TSAMBA 10-19

Akhristu oona amadziwa kufunika kokhala odzichepetsa chifukwa amatsatira chitsanzo cha Yesu. Nkhani yoyamba ikufotokoza chitsanzo cha Yesu pa nkhani ya kudzichepetsa ndipo itithandiza kuti tiziyesetsa kumutsanzira. Nkhani yachiwiri ikusonyeza zimene tingachite kuti tizikhala ngati wamng’ono.

NKHANI ZOPHUNZIRA 4, 5 TSAMBA 21-30

Nkhani zimenezi zitithandiza kudziwa kuti Yehova ndi wofunitsitsa kukhululuka ngakhale machimo akuluakulu. Nthawi zina ifeyo tingavutike kukhululukira ena. Koma mfundo za m’Malemba zingatithandize kukhala ndi mtima wokhululuka.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

8 Zochuluka Zimene Anali Nazo Zinathandiza Anthu Osowa

20 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

31 Kale Lathu

PATSAMBA LOYAMBA: Akulalikira m’katauni kakumidzi kotchedwa Albarracín kuchigawo chapakati m’dziko la Spain. Mu mpingo wa Teruel muli ofalitsa 78 ndipo m’gawo lake muli katauni ka Albarracín ndi matauni ena okwana 188

SPAIN

KULI ANTHU

47,042,900

KULI OFALITSA

111,101

OPEZEKA PA CHIKUMBUTSO MU 2012

192,942

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena