Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w12 12/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2012
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2012
w12 12/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

December 15, 2012

© 2012 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino n’ngwathu.

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA

JANUARY 28, 2013–FEBRUARY 3, 2013

Mukhoza Kukhala ndi Moyo Wabwino Kwambiri

TSAMBA 4 • NYIMBO: 115, 45

FEBRUARY 4-10, 2013

Ndinu Mtumiki Wokhulupirika

TSAMBA 9 • NYIMBO: 62, 125

FEBRUARY 11-17, 2013

Pitirizani Kukhala Monga “Anthu Osakhalitsa M’dzikoli”

TSAMBA 19 • NYIMBO: 107, 40

FEBRUARY 18-24, 2013

“Anthu Osakhalitsa M’dzikoli” Ndi Ogwirizana Polambira Mulungu

TSAMBA 24 • NYIMBO: 124, 121

CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA

NKHANI ZOPHUNZIRA 1, 2 TSAMBA 4-13

Kodi moyo wabwino umatanthauza chiyani? Nkhanizi zikusonyeza kuti yankho la funsoli ndi losiyana kwambiri ndi zimene anthu ambiri m’dzikoli angayankhe. Zikusonyezanso kuti tingakhale ndi moyo wabwino tikamakhala okhulupirika kwa Mulungu ndiponso kukwaniritsa maudindo amene watipatsa.

NKHANI ZOPHUNZIRA 3, 4 TSAMBA 19-28

Kodi Akhristu odzozedwa ndiponso anzawo a “nkhosa zina” amakhala bwanji “osakhalitsa m’dzikoli”? (Yoh. 10:16; 1 Pet. 2:11) Nkhanizi zitithandiza kudziwa yankho lake. Zitilimbikitsanso kukhalabe “osakhalitsa m’dzikoli” komanso kugwirizana ndi abale padziko lonse pogwira ntchito yolalikira.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

3 Tisamagwiritse Ntchito Baibulo Ngati Chithumwa

14 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

18 Kodi Mukukumbukira?

29 Cholinga cha Nsanja ya Olonda ya M’Chingelezi Chosavuta

32 Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda a 2012

PATSAMBA LOYAMBA: M’dziko la South Korea muli Mboni zoposa 100,000. Mboni zambiri zili m’ndende chifukwa chosalowerera ndale ndiponso kukana usilikali. Ngakhale m’ndendemo, amayesetsabe kulalikira. Ena amalalikira polemba makalata

KU SOUTH KOREA

KULI ANTHU

48,184,000

KULI OFALITSA

100,059

ABALE OMWE ANALI M’NDENDE CHAKA CHATHA

731

MWEZI ULIWONSE, ANKALALIKIRA MAOLA

9,000

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena