Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w13 4/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2013
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2013
w13 4/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

April 15, 2013

© 2013 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino n’ngwathu.

MAGAZINI YOPHUNZIRA

JUNE 3-9, 2013

Zimene Mungachite Kuti Muzipindula Powerenga Baibulo

TSAMBA 7 • NYIMBO: 114, 113

JUNE 10-16, 2013

Mawu a Mulungu Azikuthandizani Ndipo Muzithandiza Nawo Ena

TSAMBA 12 • NYIMBO: 37, 92

JUNE 17-23, 2013

“Muzitsimikizira Kuti Zinthu Zofunika Kwambiri Ndi Ziti”

TSAMBA 22 • NYIMBO: 70, 98

JUNE 24-30, 2013

Musatope Kuchita Zabwino

TSAMBA 27 • NYIMBO: 129, 63

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Zimene Mungachite Kuti Muzipindula Powerenga Baibulo

▪ Mawu a Mulungu Azikuthandizani Ndipo Muzithandiza Nawo Ena

Paulo analemba kuti: “Mawu a Mulungu ndi amoyo ndi amphamvu.” (Aheb. 4:12) Koma mphamvuyi ikhoza kutithandiza ngati timaphunzira Mawuwo ndiponso kutsatira zimene timaphunzirazo. Nkhanizi zikufotokoza zimene tingachite kuti tizipindula pophunzira Baibulo. Zikufotokozanso zimene tingachite kuti nzeru yochokera kwa Mulungu izititsogolera pa moyo wathu komanso mu utumiki.

▪ “Muzitsimikizira Kuti Zinthu Zofunika Kwambiri Ndi Ziti”

▪ Musatope Kuchita Zabwino

Ndi mwayi waukulu kukhala m’gulu la Mulungu lomwe lili ndi mbali ina padziko lapansi, ina kumwamba. Kodi tingathandize bwanji kuti ntchito ya gululi iziyenda bwino? Nanga n’chiyani chingatithandize kuti tizichita zinthu mogwirizana ndi gulu la Yehova komanso kuti tisatope? Nkhanizi ziyankha mafunso amenewa.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

3 Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Mexico

17 Tachita Utumiki wa Nthawi Zonse kwa Zaka 50 Kumpoto Kwenikweni

32 Kodi Mukudziwa?

PATSAMBA LOYAMBA: M’mipingo yambiri, abale amakumana 7:30 m’mawa kapena kum’mawa kwambiri kuti akalalikire. Iwo amayesetsa kulalikira kwa anthu amene amakumana nawo mumsewu

NEPAL

KULI ANTHU

26,620,809

KULI OFALITSA

1,667

AMACHITITSA MAPHUNZIRO A BAIBULO

3,265

[Chithunzi patsamba 2]

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena