Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w13 5/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2013
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2013
w13 5/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

May 15, 2013

© 2013 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino n’ngwathu.

MAGAZINI YOPHUNZIRA

JULY 1-7, 2013

Muzigwira Bwino Ntchito Yanu Yolalikira

TSAMBA 3 • NYIMBO: 103, 102

JULY 8-14, 2013

Kodi Ndinu “Odzipereka pa Ntchito Zabwino”?

TSAMBA 8 • NYIMBO: 108, 93

JULY 15-21, 2013

Muzilankhulana Bwino Kuti Banja Lanu Likhale Lolimba

TSAMBA 14 • NYIMBO: 36, 87

JULY 22-28, 2013

Makolo ndi Ana Ayenera Kulankhulana Mwachikondi

TSAMBA 19 • NYIMBO: 88, 3

JULY 29, 2013–AUGUST 4, 2013

Muzisankha Zinthu Mwanzeru Kuti Musataye Madalitso Anu

TSAMBA 26 • NYIMBO: 14, 134

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Muzigwira Bwino Ntchito Yanu Yolalikira

Kodi mlaliki amachita chiyani? Nkhaniyi iyankha funso limeneli ndipo ikusonyeza chifukwa chake anthu akufunikira kumva uthenga wabwino. Ikufotokozanso zimene tingachite kuti tizigwira bwino ntchito yathu yolalikira.

▪ Kodi Ndinu “Odzipereka pa Ntchito Zabwino”?

Nkhaniyi ikufotokoza mmene kukhala “odzipereka pa ntchito zabwino” kungathandizire kuti anthu ayambe kuphunzira za Mulungu. (Tito 2:14) Ikufotokoza mmene khama lathu polalikira ndiponso khalidwe lathu labwino zimathandizira.

▪ Muzilankhulana Bwino Kuti Banja Lanu Likhale Lolimba

▪ Makolo ndi Ana Ayenera Kulankhulana Mwachikondi

Mwamuna ndi mkazi ayenera kulankhulana bwino kuti azisangalala m’banja. Nkhani yoyamba ikufotokoza makhalidwe amene angatithandize kuti tizilankhulana bwino. Nkhani yachiwiri ikusonyeza zimene makolo ndi ana angachite kuti asamavutike kulankhulana bwino.

▪ Muzisankha Zinthu Mwanzeru Kuti Musataye Madalitso Anu

Kodi Akhristu ali ndi madalitso ati? Kodi tingaphunzire zotani zokhudza madalitsowo pa zimene Esau anachita? Kodi ndi zinthu ziti zimene zingatithandize kusankha mwanzeru pa nkhani zokhudza madalitso athu? Mafunso amenewa ayankhidwa m’nkhaniyi.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

13 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

24 Zimene Zatithandiza Kukhalabe Osangalala

31 Kale Lathu

PATSAMBA LOYAMBA: Alongowa ali ku London ndipo akulalikira kwa mwinisitolo pogwiritsa ntchito kabuku ka m’chinenero cha Chigujarati

LONDON KU ENGLAND

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena