Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w13 7/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2013
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2013
w13 7/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

July 15, 2013

© 2013 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino n’ngwathu.

MAGAZINI YOPHUNZIRA

SEPTEMBER 2-8, 2013

“Tiuzeni, Kodi Zinthu Zimenezi Zidzachitika Liti?”

TSAMBA 3 • NYIMBO: 128, 101

SEPTEMBER 9-15, 2013

“Dziwani Kuti Ine Ndili Pamodzi ndi Inu Masiku Onse”

TSAMBA 9 • NYIMBO: 30, 109

SEPTEMBER 16-22, 2013

Yesu Amadyetsa Anthu Ambiri Kudzera mwa Anthu Ochepa

TSAMBA 15 • NYIMBO: 108, 117

SEPTEMBER 23-29, 2013

“Ndani Kwenikweni Amene Ali Kapolo Wokhulupirika ndi Wanzeru?”

TSAMBA 20 • NYIMBO: 107, 116

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ “Tiuzeni, Kodi Zinthu Zimenezi Zidzachitika Liti?”

▪ “Dziwani Kuti Ine Ndili Pamodzi ndi Inu Masiku Onse”

Nkhani zimenezi zikufotokoza mavesi ena a Mateyu chaputala 24 ndi 25. Zikusintha zinthu zina zimene tinkakhulupirira zokhudza nthawi imene ulosi wa Yesu wonena za masiku otsiriza ndiponso wokhudza tirigu ndi namsongole, uyenera kukwaniritsidwa. Nkhanizi zikufotokozanso mmene kusintha kumeneku kungatithandizire.

▪ Yesu Amadyetsa Anthu Ambiri Kudzera mwa Anthu Ochepa

▪ “Ndani Kwenikweni Amene Ali Kapolo Wokhulupirika ndi Wanzeru?”

Yesu ankadyetsa anthu ambiri kudzera mwa anthu ochepa. Ankachita zimenezi podyetsa khamu la anthu mozizwitsa komanso popereka chakudya chauzimu kwa otsatira ake. Nkhani yoyamba ikufotokoza za anthu ochepa amene ankawagwiritsa ntchito podyetsa Akhristu oyambirira. Nkhani yachiwiri ikufotokoza za anthu ochepa amene Khristu akuwagwiritsa ntchito potidyetsa masiku ano.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

26 M’bale Watsopano M’Bungwe Lolamulira

27 Timasangalala Kutumikira Yehova Kwina Kulikonse

32 “Zithunzi Zokongola Kwambiri”

PATSAMBA LOYAMBA: Akulalikira kunyumba ndi nyumba ku Bukimba, m’dera la Runda m’dziko la Rwanda

RWANDA

Wa Mboni mmodzi pa anayi alionse m’dzikoli akuchita upainiya. A Mboni ena onse akhama amalalikira maola pafupifupi 20 mwezi uliwonse.

MBONI

22,734

MAPHUNZIRO A BAIBULO

52,123

OPEZEKA PA CHIKUMBUTSO MU 2012

69,582

[Chithunzi patsamba 2]

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena