Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w13 9/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2013
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2013
w13 9/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

September 15, 2013

© 2013 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino n’ngwathu.

MAGAZINI YOPHUNZIRA

OCTOBER 28, 2013–NOVEMBER 3, 2013

Zikumbutso za Yehova Ndi Zodalirika

TSAMBA 7 • NYIMBO: 64, 114

NOVEMBER 4-10, 2013

Kodi Zikumbutso za Yehova Zimakondweretsa Mtima Wanu?

TSAMBA 12 • NYIMBO: 116, 52

NOVEMBER 11-17, 2013

Kodi Mwasandulika?

TSAMBA 17 • NYIMBO: 69, 106

NOVEMBER 18-24, 2013

Muzisankha Zochita Mwanzeru

TSAMBA 22 • NYIMBO: 27, 83

NOVEMBER 25, 2013–DECEMBER 1, 2013

Upainiya Umalimbitsa Ubwenzi Wathu ndi Mulungu

TSAMBA 27 • NYIMBO: 95, 104

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Zikumbutso za Yehova Ndi Zodalirika

▪ Kodi Zikumbutso za Yehova Zimakondweretsa Mtima Wanu?

Yehova wakhala akugwiritsa ntchito zikumbutso zake potsogolera anthu ake. Kodi zikumbutso zakezo n’chiyani? Nkhani yoyamba ikufotokoza chifukwa chake tiyenera kukhulupirira zikumbutso za Mulungu. Yachiwiri ikufotokoza zinthu zitatu zimene zingatithandize kukhulupirira kwambiri zikumbutso za Yehova.

▪ Kodi Mwasandulika?

▪ Muzisankha Zochita Mwanzeru

Anthufe timachita zinthu mogwirizana ndi mmene tinakulira ndi kumene timakhala. Kodi tingatani kuti tizisankha zochita mogwirizana ndi zimene Mulungu amafuna? Nanga n’chiyani chingatithandize kuti tichitedi zimene tasankha? Nkhani ziwirizi zitithandiza kudzifufuza bwinobwino pa nkhaniyi.

▪ Upainiya Umalimbitsa Ubwenzi Wathu ndi Mulungu

M’nkhaniyi tiona zinthu 8 zimene zingatithandize kulimbitsa ubwenzi wathu ndi Yehova tikamachita upainiya. Ngati panopa mukuchita upainiya, kodi n’chiyani chingakuthandizeni kupitiriza ngakhale mutakumana ndi mavuto? Nanga mungatani ngati mukufuna kuchita upainiya ndi kulandira madalitso ake?

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

3 Kusiyanitsa Zinthu N’kothandiza Kwambiri

32 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

PATSAMBA LOYAMBA: Abale ndi alongo a kudera la Amazonas, kumpoto kwa dziko la Peru, amagwiritsa ntchito mpata uliwonse kuti alalikire

PERU

KULI ANTHU OKWANA

29,734,000

KULI OFALITSA OKWANA

117,245

ANTHU AMENE ABATIZIDWA PA ZAKA 5 ZAPITAZI

28,824

M’dziko la Peru, amamasulira mabuku athu m’zinenero 6. Kuli apainiya apadera ndiponso amishonale oposa 120 amene amalalikira m’zinenero zina osati Chisipanishi chokha

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena