Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w13 10/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2013
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2013
w13 10/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

October 15, 2013

© 2013 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania.

MAGAZINI YOPHUNZIRA

DECEMBER 2-8, 2013

Chilengedwe Chimatithandiza Kukhulupirira Kwambiri Mulungu

TSAMBA 7 • NYIMBO: 110, 15

DECEMBER 9-15, 2013

“Tumikirani Yehova Monga Akapolo”

TSAMBA 12 • NYIMBO: 62, 84

DECEMBER 16-22, 2013

Kodi Tikuphunzira Chiyani pa Pemphero Limene Linakonzedwa Bwino?

TSAMBA 21 • NYIMBO: 68, 6

DECEMBER 23-29, 2013

Muzichita Zinthu Mogwirizana ndi Pemphero la Yesu

TSAMBA 26 • NYIMBO: 57, 56

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Chilengedwe Chimatithandiza Kukhulupirira Kwambiri Mulungu

Mulungu amene sitingathe kumuona analenga zinthu zonse zimene timatha kuziona. Kodi mumakhulupirira zimenezi ndi mtima wanu wonse? Koma anthu ena sakhulupirira zimenezi. Kodi anthu otero tingawathandize bwanji kudziwa zoona zenizeni zokhudza Mlengi kwinaku tikulimbitsa chikhulupiriro chathu? Nkhani ino itithandiza kuyankha funso limeneli.

▪ “Tumikirani Yehova Monga Akapolo”

Akhristu akulimbikitsidwa kutumikira Yehova monga akapolo. M’nkhaniyi tiona zimene Chilamulo cha Mose chinanena zokhudza akapolo ndiponso zimene tingachite kuti tipewe kukhala akapolo a Satana ndi zinthu zokopa za m’dzikoli. Komanso tiona ubwino wotumikira Mulungu mokhulupirika ngati akapolo.

▪ Kodi Tikuphunzira Chiyani pa Pemphero Limene Linakonzedwa Bwino?

▪ Muzichita Zinthu Mogwirizana ndi Pemphero la Yesu

Tikamaganizira Mawu a Mulungu mozama tsiku ndi tsiku, mapemphero athu adzakhala ogwira mtima. Umu ndi mmene zinalili pamene Alevi anapemphera m’malo mwa anthu a Mulungu. Nkhani yachiwiri ikusonyeza mmene tingachitire zinthu mogwirizana ndi pemphero lina la Yesu. Mapemphero onsewa akusonyeza ubwino woika patsogolo zofuna za Yehova osati zofuna zathu.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

3 Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Philippines

17 Tadalitsidwa Chifukwa Chodalira Yehova

31 Kodi Mungatani Kuti Muchenjeze Anthu Ambiri?

PATSAMBA LOYAMBA: M’bale akulalikira ku Panajachel, tauni yaing’ono imene ili m’mphepete mwa nyanja ya Atitlan. Kuwonjezera pa Chisipanishi, Mboni za Yehova ku Guatemala zimalalikira uthenga wabwino m’zinenero 11

GUATEMALA

KULI ANTHU OKWANA:

15,169,000

KULI OFALITSA OKWANA:

34,693

MAPHUNZIRO A BAIBULO:

47,606

[Chithunzi patsamba 2]

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena