Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w13 11/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2013
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2013
w13 11/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

November 15, 2013

© 2013 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania.

MAGAZINI YOPHUNZIRA

DECEMBER 30, 2013–JANUARY 5, 2014

“Khalani Maso Kuti Musanyalanyaze Kupemphera”

TSAMBA 3 • NYIMBO: 67, 81

JANUARY 6-12, 2014

Pitirizani ‘Kuyembekezera Moleza Mtima’

TSAMBA 10 • NYIMBO: 119, 32

JANUARY 13-19, 2014

Kodi Abusa 7 ndi Atsogoleri 8 Akuimira Ndani Masiku Ano?

TSAMBA 16 • NYIMBO: 43, 123

JANUARY 20-26, 2014

Muzimvera Abusa Amene Yehova Watipatsa

TSAMBA 21 • NYIMBO: 125, 122

JANUARY 27, 2014–FEBRUARY 2, 2014

Abusa, Tsanzirani Abusa Aakulu

TSAMBA 26 • NYIMBO: 5, 84

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ “Khalani Maso Kuti Musanyalanyaze Kupemphera”

Pamene mapeto a dziko loipa la Satanali akuyandikira, tiyenera kuyesetsa kukhala maso mwauzimu. M’nkhani ino tiona kuti kuchita khama popemphera kungatithandize kuchita zimenezi.

▪ Pitirizani ‘Kuyembekezera Moleza Mtima’

M’nkhani ino tiona zimene tingaphunzire pa chitsanzo cha mneneri Mika pa nkhani ya kuleza mtima. Tionanso zimene zidzasonyeze kuti Yehova watsala pang’ono kuwononga dziko loipali. Komanso tiona zimene tingachite posonyeza kuti timayamikira kuleza mtima kwa Mulungu.

▪ Kodi Abusa 7 ndi Atsogoleri 8 Akuimira Ndani Masiku Ano?

Tingaphunzire zambiri pa zimene zinachitika Senakeribu ataukira Yerusalemu m’nthawi ya Hezekiya. Nkhaniyi ingathandize kwambiri akulu amene apatsidwa udindo woweta nkhosa za Mulungu.

▪ Muzimvera Abusa Amene Yehova Watipatsa

▪ Abusa, Tsanzirani Abusa Aakulu

Nkhani yoyamba ikufotokoza mmene Yehova ndi Yesu amawetera nkhosa zawo zapadziko lapansi masiku ano komanso zimene nkhosazo ziyenera kuchita. Nkhani yachiwiri ikufotokoza mtima umene akulu ayenera kusonyeza pamene akuweta nkhosa za Mulungu monga abusa aang’ono.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

8 Kodi Tingathandize Bwanji Anthu Ena?

15 Kutumikira Mulungu Kuli Ngati Mankhwala Ake

31 Kale Lathu

PATSAMBA LOYAMBA: Akulalikira mumsewu pasiteshoni ya sitima ku Tokyo. Anthu oposa 2.8 miliyoni amapita ku Tokyo tsiku lililonse kukagwira ntchito. Choncho abale ndi alongo akuyesetsa kulalikira kwa anthu amene sapezeka pakhomo

JAPAN

KULI ANTHU OKWANA:

126,536,000

KULI OFALITSA OKWANA:

216,692

APAINIYA OKHAZIKIKA:

65,245

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena