Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w14 2/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2014
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2014
w14 2/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

February 15, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania.

NKHANI ZOPHUNZIRA

APRIL 7-13, 2014

Tamandani Khristu, Mfumu Yaulemerero

TSAMBA 3 • NYIMBO: 99, 107

APRIL 14-20, 2014

Sangalalani Chifukwa cha Ukwati wa Mwanawankhosa

TSAMBA 8 • NYIMBO: 109, 100

APRIL 21-27, 2014

Yehova Amatipatsa Zinthu Zofunika Ndipo Amatiteteza

TSAMBA 16 • NYIMBO: 60, 51

APRIL 28, 2014–MAY 4, 2014

Yehova Ndi Mnzathu Weniweni

TSAMBA 21 • NYIMBO: 91, 63

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Tamandani Khristu, Mfumu Yaulemerero

▪ Sangalalani Chifukwa cha Ukwati wa Mwanawankhosa

Yesu Khristu, yemwe ndi Mfumu, anamangirira lupanga lake n’kukwera pahatchi kuti akagonjetse adani ake. Akamaliza kuwagonjetsa adzakwatira mkazi wokongola woperekezedwa ndi anamwali anzake. Nkhani yosangalatsayi yafotokozedwa mu Salimo 45. Werengani kuti muone mmene nkhaniyi ikukukhudzirani.

▪ Yehova Amatipatsa Zinthu Zofunika Ndipo Amatiteteza

▪ Yehova Ndi Mnzathu Weniweni

N’chiyani chingatithandize kuti tiziona kuti Yehova ndi Atate wathu wakumwamba? Nkhanizi zitithandiza kuti tizigwirizana kwambiri ndi Yehova, yemwe amatipatsa zofunika, amatiteteza komanso ndi Mnzathu weniweni. Zitilimbikitsanso kuti tizithandiza ena kuti ayambe kumulemekeza.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

13 Mkazi Wamasiye wa ku Zarefati Anadalitsidwa Chifukwa cha Chikhulupiriro

26 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

28 ‘Tiziona Ubwino wa Yehova’

30 Kale Lathu

PATSAMBA LOYAMBA: Pamalo awa (Michaelerplatz) mumzinda wa Vienna pamapezeka anthu ambiri ndipo ndi malo abwino kulalikirapo uthenga wa m’Baibulo. Mlongoyu akulalikira m’Chitchainizi ndipo akugawira buku lakuti, Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni?

AUSTRIA

KULI OFALITSA OKWANA

20,923

APAINIYA

2,201

MAPHUNZIRO A BAIBULO

10,987

Mumzindawu uthenga wabwino wa Ufumu umalalikidwa m’zinenero 25

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena