Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w14 4/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2014
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2014
w14 4/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

April 15, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

JUNE 2-8, 2014

Tsanzirani Chikhulupiriro cha Mose

TSAMBA 3 • NYIMBO: 33, 133

JUNE 9-15, 2014

Kodi ‘Mukuona Wosaonekayo’?

TSAMBA 8 • NYIMBO: 81, 132

JUNE 16-22, 2014

Simungatumikire Ambuye Awiri

TSAMBA 17 • NYIMBO: 62, 106

JUNE 23-29, 2014

Limbani Mtima, Yehova Akuthandizani

TSAMBA 22 • NYIMBO: 22, 95

JUNE 30, 2014–JULY 6, 2014

Yehova Amaona Mavuto Athu N’kutithandiza

TSAMBA 27 • NYIMBO: 69, 120

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Tsanzirani Chikhulupiriro cha Mose

▪ Kodi ‘Mukuona Wosaonekayo’?

Mwa chikhulupiriro, Mose ankatha kuona zinthu zosaoneka. Nkhani ziwirizi zikufotokoza mmene ifeyo tingasonyezere chikhulupiriro ngati Mose n’kupitiriza “kupirira moleza mtima ngati kuti tikuona Wosaonekayo.”—Aheb. 11:27.

▪ Simungatumikire Ambuye Awiri

▪ Limbani Mtima, Yehova Akuthandizani

Anthu ambirimbiri padziko lonse akupita m’mayiko ena kukafuna ntchito. Ambiri amasiya amuna kapena akazi awo komanso ana. Nkhanizi zitithandiza kumvetsa zimene Yehova akufuna kuti tizichita pokwaniritsa udindo wathu wosamalira banja komanso mmene amatithandizira kuti tikwaniritse udindo umenewu.

▪ Yehova Amaona Mavuto Athu N’kutithandiza

Tikamawerenga mawu akuti “maso a Yehova ali paliponse,” ena amaganiza kuti Mulungu amatiyang’anitsitsa kuti aone zimene tikulakwitsa n’kutilanga. Zimenezi zimachititsa kuti asamafune kumutumikira. (Miy. 15:3) Koma nkhaniyi itithandiza kuona njira 5 zosonyeza mmene timapindulira, Yehova akamatiyang’ana.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

13 Madalitso Amene Ndapeza mu Utumiki wa Nthawi Zonse

13 Kodi Mukudziwa?

PATSAMBA LOYAMBA: M’bale akulalikira kwa munthu amene akumumeta tsitsi ku Istanbul, ndipo akum’patsa kabuku kakuti Uthenga Wabwino

TURKEY

KULI ANTHU OKWANA

75,627,384

KULI OFALITSA OKWANA

2,312

MAPHUNZIRO A BAIBULO

1,632

WOFALITSA ALIYENSE

Ayenera kulalikira anthu 32,711

Kuchokera mu 2004 chiwerengero cha apainiya okhazikika ku Turkey chawonjezeka ndi 165%

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena