Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w14 5/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2014
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2014
w14 5/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

May 15, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

JULY 7-13, 2014

Kodi ‘Tingayankhe Bwanji Wina Aliyense’?

TSAMBA 6 • NYIMBO: 96, 93

JULY 14-20, 2014

Muzichitira Anthu Zimene Mungafune Kuti Akuchitireni

TSAMBA 11 • NYIMBO: 73, 98

JULY 21-27, 2014

Yehova Ndi Mulungu Wadongosolo

TSAMBA 21 • NYIMBO: 125, 53

JULY 28, 2014–AUGUST 3, 2014

Kodi Mukuyenda Limodzi ndi Gulu la Yehova?

TSAMBA 26 • NYIMBO: 45, 27

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Kodi ‘Tingayankhe Bwanji Wina Aliyense’?

▪ Muzichitira Anthu Zimene Mungafune Kuti Akuchitireni

Nthawi zina anthu amatifunsa mafunso ovuta mu utumiki. Nkhani yoyamba itithandiza kudziwa zinthu zitatu zimene tingachite kuti tiziwayankha mogwira mtima. (Akol. 4:6) Nkhani yachiwiri ikusonyeza kufunika kotsatira mawu a Yesu a pa Mateyu 7:12 tikamalalikira.

▪ Yehova Ndi Mulungu Wadongosolo

▪ Kodi Mukuyenda Limodzi ndi Gulu la Yehova?

Yehova wakhala akuthandiza atumiki ake kuchita zinthu mwadongosolo. Nkhani ziwirizi zikusonyeza zimene Mulungu amafuna kuti tizichita. Ikusonyezanso chifukwa chake tiyenera kuyenda limodzi ndi gulu la Yehova masiku ano.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

3 ‘Chakudya Changa N’kuchita Chifuniro cha Mulungu’

16 Yehova Wandithandiza Kwambiri

31 Kale Lathu

PATSAMBA LOYAMBA: Akulalikira kumsika wa nsomba. Anthu a pachilumbachi amalankhula zilankhulo zoposa 20

SAIPAN

KULI ANTHU

48,220

KULI OFALITSA

201

KULI APAINIYA OKHAZIKIKA

32

KULI APAINIYA OTHANDIZA

76

Opezeka pa Chikumbutso mu 2013 analipo 570

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena