Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w14 6/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2014
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2014
w14 6/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

June 15, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

AUGUST 4-10, 2014

“Uzikonda Yehova Mulungu Wako”

TSAMBA 12 • NYIMBO: 3, 65

AUGUST 11-17, 2014

“Uzikonda Mnzako Mmene Umadzikondera Wekha”

TSAMBA 17 • NYIMBO: 84, 72

AUGUST 18-24, 2014

Kodi Mumaona Anthu Ofooka Mmene Yehova Amawaonera?

TSAMBA 23 • NYIMBO: 77, 79

AUGUST 25-31, 2014

Thandizani Ena Kuti Azichita Zonse Zimene Angathe

TSAMBA 28 • NYIMBO: 42, 124

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ “Uzikonda Yehova Mulungu Wako”

▪ “Uzikonda Mnzako Mmene Umadzikondera Wekha”

Nkhani ziwirizi zikufotokoza malamulo awiri aakulu a m’Chilamulo amene Yesu Khristu ananena. Onani zimene Yesu ankatanthauza ponena kuti tizikonda Yehova ndi mtima wathu wonse, moyo wathu wonse komanso maganizo athu onse. Onaninso mmene tingasonyezere kuti timakonda anzathu mmene timadzikondera.

▪ Kodi Mumaona Anthu Ofooka MmeneYehova Amawaonera?

▪ Thandizani Ena Kuti Azichita ZonseZimene Angathe

Kodi tingathandize bwanji anthu amene afooka? Nkhani yoyamba ikuyankha funso limeneli. Nkhani yachiwiri ikufotokoza zimene tingachite pothandiza abale achinyamata komanso atsopano kuti azichita zonse zimene angathe.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

3 “Salaza Njira ya Phazi Lako” Kuti Uyende Bwino

7 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

8 Kodi Tingathandize Bwanji Akhristu Amene Banja Lawo Latha?

22 Kodi Mukukumbukira?

PATSAMBA LOYAMBA: Akulalikira kwa msodzi wolankhula Chimbukushu m’mphepete mwa mtsinje wa Okavango

BOTSWANA

KULI ANTHU

2,021,000

KULI OFALITSA

2,096

KULI MIPINGO

47

OPEZEKA PA CHIKUMBUTSO MU 2013

5,735

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena