Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w14 7/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2014
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2014
w14 7/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

July 15, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

SEPTEMBER 1-7, 2014

“Yehova Amadziwa Anthu Ake”

TSAMBA 7 • NYIMBO: 63, 66

SEPTEMBER 8-14, 2014

Anthu a Yehova Amakana Kuchita Zosalungama

TSAMBA 12 • NYIMBO: 64, 61

SEPTEMBER 15-21, 2014

“Inu Ndinu Mboni Zanga”

TSAMBA 23 • NYIMBO: 31, 92

SEPTEMBER 22-28, 2014

“Mudzakhala Mboni Zanga”

TSAMBA 28 • NYIMBO: 102, 103

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ “Yehova Amadziwa Anthu Ake”

▪ Anthu a Yehova Amakana Kuchita Zosalungama

Nkhanizi zikufotokoza tanthauzo la lemba la 2 Timoteyo 2:19. Zikusonyezanso kuti lembali likugwirizana ndi zimene zinachitika m’nthawi ya Mose. Zitithandiza kudziwa mmene tingasonyezere kuti ndife ‘anthu a Yehova’ ndiponso kuti timakana kuchita zosalungama.

▪ “Inu Ndinu Mboni Zanga”

▪ “Mudzakhala Mboni Zanga”

M’nkhanizi tiona chifukwa chake timatchedwa Mboni za Yehova. Tiyenera kuchita khama pa ntchito yolalikira za Yehova ndi Yesu komanso kukhala ndi khalidwe loyera limene limawalemekeza.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

3 Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Micronesia

17 Bambo Anga Anamwalira Koma Ndinapeza Bambo Ena

PATSAMBA LOYAMBA: Alongo awiri akugwiritsa ntchito buku la Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni? polalikira azimayi awiri achindewele. Azimayiwa avala mmene Andewele amavalira ndipo nyumbayo ndi mmene nyumba za kumidzi yawo zimaonekera. Ku South Africa, anthu awiri okha pa anthu 100 alionse ndi Andewele

SOUTH AFRICA

KULI ANTHU

50,500,000

KULI OFALITSA

94,101

OFALITSA OLANKHULA CHINDEWELE

1,003

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena