Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w15 2/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 2/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

February 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

APRIL 6-12, 2015

Khalani Odzichepetsa Ndiponso Achifundo Ngati Yesu

TSAMBA 5 • NYIMBO: 5, 84

APRIL 13-19, 2015

Khalani Olimba Mtima Ndiponso Ozindikira Ngati Yesu

TSAMBA 10 • NYIMBO: 99, 108

APRIL 20-26, 2015

Zinthu Zimene Zinathandiza Kuti Anthu Aphunzire za Yehova

TSAMBA 19 • NYIMBO: 98, 104

APRIL 27, 2015–MAY 3, 2015

Yehova Akutsogolera Ntchito Yolalikira Padziko Lonse

TSAMBA 24 • NYIMBO: 103, 66

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Khalani Odzichepetsa Ndiponso Achifundo Ngati Yesu

▪ Khalani Olimba Mtima Ndiponso Ozindikira Ngati Yesu

Baibulo limatilimbikitsa kutsatira mapazi a Yesu mosamala. (1 Pet. 2:21) Koma kodi anthu ochimwafe tingatsatiredi chitsanzo cha Yesu? Nkhani yoyamba ikufotokoza zimene tingachite kuti tikhale odzichepetsa ndiponso achifundo ngati Yesu. Nkhani yachiwiri ikusonyeza zimene tingachite kuti tikhale olimba mtima ndiponso ozindikira ngati Yesu.

▪ Zinthu Zimene Zinathandiza Kuti Anthu Aphunzire za Yehova

▪ Yehova Akutsogolera Ntchito Yolalikira Padziko Lonse

Nkhani yoyamba ikusonyeza zimene Yehova anachita pothandiza Akhristu oyambirira kuti azilalikira uthenga wabwino. M’nkhani yachiwiri tidzakambirana zinthu za masiku ano zimene zimatithandiza kuti tizilalikira uthenga wa Ufumu kwa anthu amtima wabwino padziko lonse lapansi.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

3 Anthu a ku Japan Analandira Mphatso

15 Kodi Tingatani Kuti Tizikondabe Kulalikira?

29 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

31 Kale Lathu

PATSAMBA LOYAMBA: Akulalikira kunyumba ndi nyumba pachilumba cha Bali ndipo akugawira Galamukani! kwa munthu amene wawalandira bwino

INDONESIA

KULI ANTHU

237,600,000

KULI OFALITSA

24,521

KULI APAINIYA OKHAZIKIKA

2,472

Apainiya apadera 369 akutumikira m’zilumba 28 za m’dzikoli

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena