Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w15 3/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 3/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

March 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

MAY 4-10, 2015

“Munavomereza Kuti Zimenezi Zichitike”

TSAMBA 7 • NYIMBO: 65, 64

MAY 11-17, 2015

Kodi ‘Mudzakhalabe Maso’?

TSAMBA 12 • NYIMBO: 108, 24

MAY 18-24, 2015

Kodi Tikuphunzira Chiyani pa Fanizo la Matalente?

TSAMBA 19 • NYIMBO: 101, 116

MAY 25-31, 2015

Tizithandiza Abale a Khristu Mokhulupirika

TSAMBA 25 • NYIMBO: 107, 63

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ “Munavomereza Kuti Zimenezi Zichitike”

▪ Kodi ‘Mudzakhalabe Maso’?

Nkhani yoyamba ikufotokoza kuti Yehova akutsogolera anthu powaphunzitsa m’njira yosavuta. Nkhani yachiwiri ikufotokoza fanizo la Yesu la anamwali 10. Fanizoli lingatithandize kukhalabe maso masiku ano.

▪ Kodi Tikuphunzira Chiyani pa Fanizo la Matalente?

▪ Tizithandiza Abale a Khristu Mokhulupirika

Nkhanizi zikufotokoza mafanizo awiri amene Yesu anapereka pofotokoza chizindikiro cha kukhalapo kwake. Fanizo limodzi ndi lokhudza akapolo amene anapatsidwa matalente ndipo lina ndi loti anthu adzasiyanitsidwa ngati nkhosa ndi mbuzi. M’nkhanizi tiziyankha funso lakuti: N’chifukwa chiyani Yesu anapereka fanizoli ndipo likutithandiza bwanji?

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

3 Tinapeza Ntchito Yabwino Kwambiri

17 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

30 Kodi N’zothekadi Kukwatira Kapena Kukwatiwa “Mwa Ambuye”?

PATSAMBA LOYAMBA: Anthu ambiri amapita ku Honduras kukaona mabwinja a ku Copán ndipo a Mboni za Yehova akuthandiza anthuwa kuti aziganizira zam’tsogolo

HONDURAS

KULI ANTHU

8,111,000

KULI OFALITSA

22,098

KULI APAINIYA OKHAZIKIKA

3,471

M’dzikoli, anthu ambiri amalankhula Chisipanishi. Koma kuli ofalitsa 365 m’mipingo 12 amene amagwiritsa ntchito chilankhulo cha Chigarifuna. Chilankhulo chamanja cha kumeneko chimagwiritsidwanso ntchito m’mipingo 11 ndi timagulu titatu

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena