Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w15 4/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 4/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

April 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

JUNE 1-7, 2015

Kodi Mumaphunzitsa Ena Kuti Akhalenso Akulu?

TSAMBA 3 • NYIMBO: 123, 121

JUNE 8-14, 2015

Zimene Mungachite Pophunzitsa Ena Kuti Akhale Akulu

TSAMBA 9 • NYIMBO: 45, 70

JUNE 15-21, 2015

Kodi Yehova Ndi Mnzanu Weniweni?

TSAMBA 19 • NYIMBO: 91, 11

JUNE 22-28, 2015

Muzikhulupirira Yehova Nthawi Zonse

TSAMBA 24 • NYIMBO: 106, 49

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Kodi Mumaphunzitsa Ena Kuti Akhalenso Akulu?

▪ Zimene Mungachite Pophunzitsa Ena Kuti Akhale Akulu

N’chifukwa chiyani akulu ayenera kuphunzitsa ena kuti akhalenso akulu? Kodi angawaphunzitse bwanji? Kodi akulu komanso anthu amene akuphunzitsidwawo angaphunzire chiyani kwa Samueli, Eliya ndiponso Elisa? Nkhani ziwirizi ziyankha mafunso amenewa.

▪ Kodi Yehova Ndi Mnzanu Weniweni?

▪ Muzikhulupirira Yehova Nthawi Zonse

Ubwenzi wabwino ndi Yehova ungatithandize kuti tipirire vuto lililonse. Nkhani ziwirizi zikusonyeza zimene tingachite kuti tikhale pa ubwenzi wabwino ndi Yehova. Choyamba tiyenera kulankhulana naye ndipo chachiwiri tiyenera kumukhulupirira nthawi zonse.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

14 Ndadalitsidwa “M’nthawi Yabwino ndi M’nthawi Yovuta”

29 Kuchotsa Anthu Osalapa Kumathandiza

32 Mtengo Ukadulidwa Umaphukanso

PATSAMBA LOYAMBA: Mkulu akuphunzitsa m’bale kulalikira pogwiritsa ntchito shelefu yamatayala m’mphepete mwa msewu wa Haiphong ku Kowloon

HONG KONG

KULI ANTHU

7,234,800

KULI OFALITSA

5,747

MAPHUNZIRO A BAIBULO

6,382
Chithunzi patsamba 2
180,000+

Gulu limapeza zinthu monga mashelefu ndi matebulo zoposa 180,000 kudzera ku ofesi ya nthambi ya ku Hong Kong n’kutumiza m’mayiko osiyanasiyana

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena