Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w15 5/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 5/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

May 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

JUNE 29, 2015–JULY 5, 2015

Khalani Maso, Satana Akufuna Kukumezani

TSAMBA 9 • NYIMBO: 54, 43

JULY 6-12, 2015

N’zotheka Kugonjetsa Satana

TSAMBA 14 • NYIMBO: 60, 100

JULY 13-19, 2015

Ankaona Malonjezo Ali Patali

TSAMBA 19 • NYIMBO: 81, 134

JULY 20-26, 2015

Tsanzirani Amene Wakulonjezani Moyo Wosatha

TSAMBA 24 • NYIMBO: 12, 69

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Khalani Maso, Satana Akufuna Kukumezani

▪ N’zotheka Kugonjetsa Satana

M’Baibulo, Satana amayerekezeredwa ndi mkango wobangula umene ukufunafuna nyama. Iye ndi wamphamvu, wolusa komanso wachinyengo. Nkhanizi zikusonyeza kuti tiyenera kusamala kwambiri kuti asativulaze. Itithandizanso kudziwa zimene tiyenera kuchita kuti titetezeke ku misampha yake.

▪ Ankaona Malonjezo Ali Patali

▪ Tsanzirani Amene Wakulonjezani Moyo Wosatha

Anthufe tili ndi luso lotha kuona m’maganizo mwathu zinthu zimene sitinazionepo. Luso limeneli tikhoza kuligwiritsa ntchito mwanzeru kapena mopanda nzeru. M’nkhanizi tiona zimene tingaphunzire kwa anthu angapo otchulidwa m’Baibulo. Tiona mmene tingagwiritsire ntchito luso loona zinthu m’maganizo mwathu kuti titsanzire makhalidwe a Yehova monga chikondi, chifundo, nzeru ndi chimwemwe.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

3 Chikondi Changa cha Poyamba Chandithandiza Kupirira

29 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

31 Kale Lathu

PATSAMBA LOYAMBA: Abale awiri akuchititsa phunziro la Baibulo

ARMENIA

KULI ANTHU

3,026,900

KULI OFALITSA

11,143

APAINIYA OKHAZIKIKA

2,205
23,844

Opezeka pa Chikumbutso pa April 14, 2014. Anthuwa ndi ambiri tikayerekezera ndi chiwerengero cha ofalitsa

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena