Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w15 10/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 10/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

October 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

NOVEMBER 30, 2015–DECEMBER 6, 2015

Kodi Mumaona Dzanja la Mulungu Likukuthandizani?

TSAMBA 4

DECEMBER 7-13, 2015

“Tiwonjezereni Chikhulupiriro”

TSAMBA 9

DECEMBER 14-20, 2015

Tisalole Chilichonse Kutisokoneza Potumikira Yehova

TSAMBA 18

DECEMBER 21-27, 2015

Tiziganizira Kwambiri za Yehova

TSAMBA 23

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Kodi Mumaona Dzanja la Mulungu Likukuthandizani?

▪ “Tiwonjezereni Chikhulupiriro”

M’nkhani yoyamba tikambirana umboni woti Yehova amatikonda komanso kutithandiza. Zimenezi zitithandiza kuti tisakhale ngati anthu amene amalakwitsa zinthu chifukwa chosazindikira zimene Yehova akuchita. Nkhani yachiwiri ikusonyeza kuti chikhulupiriro n’chofunika kwambiri kuti tidzapulumuke ndipo tikambirana zimene tingachite kuti tikhale ndi chikhulupiriro cholimba.—Aheb. 11:6.

▪ Tisalole Chilichonse Kutisokoneza Potumikira Yehova

▪ Tiziganizira Kwambiri za Yehova

Masiku ano pali zinthu zambiri zimene zingatisokoneze potumikira Yehova. Koma kodi tingatani kuti zinthu zimenezi zisatisokoneze? Nanga tingatani kuti tizimvetsa komanso kukumbukira zimene timawerenga m’Mawu a Mulungu? Nkhani ziwirizi zikuyankha mafunso amenewa.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

3 Tizilemekeza Kwambiri Abale Ngati Amenewa

14 Sananong’oneze Bondo ndi Zimene Anasankha Ali Mnyamata

28 Kuyandikira kwa Mulungu Ndi Kwabwino

30 ‘Munthu Wosadziwa Zinthu Amakhulupirira Mawu Alionse’

PATSAMBA LOYAMBA: M’bale akuchititsa msonkhano wokonzekera utumiki m’katauni kotchedwa St. Helens, ku Tasmania

TASMANIA, KU AUSTRALIA

KULI ANTHU

514,800

KULI MIPINGO

24

KULI OFALITSA

1,779

WOFALITSA ALIYENSE AYENERA KULALIKIRA ANTHU

289

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena