Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w15 11/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 11/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

November 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

DECEMBER 28, 2015–JANUARY 3, 2016

Muziphunzitsa Ana Anu Aang’ono Kuti Azitumikira Yehova

TSAMBA 3

JANUARY 4-10, 2016

Muziphunzitsa Ana Anu Achinyamata Kuti Azitumikira Yehova

TSAMBA 8

JANUARY 11-17, 2016

Yehova Ndi Mulungu Wachikondi

TSAMBA 16

JANUARY 18-24, 2016

Kodi ‘Mumakonda Anzanu Ngati Mmene Mumadzikondera Nokha’?

TSAMBA 21

JANUARY 25-31, 2016

Zimene Zachitika M’zaka 100 Zimene Ufumu Wakhala Ukulamulira

TSAMBA 26

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Muziphunzitsa Ana Anu Aang’ono Kuti Azitumikira Yehova

▪ Muziphunzitsa Ana Anu Achinyamata Kuti Azitumikira Yehova

Yehova anapatsa makolo udindo wofunika kwambiri wophunzitsa ana awo kuti azimutumikira. Nkhani ziwirizi zikufotokoza zimene makolo angachite kuti azitsanzira Yesu pophunzitsa ana awo mwachikondi, modzichepetsa ndiponso mozindikira.

▪ Yehova Ndi Mulungu Wachikondi

▪ Kodi ‘Mumakonda Anzanu Ngati Mmene Mumadzikondera Nokha’?

Nkhani yoyamba ikusonyeza kuti Yehova ndi Mulungu wachikondi. Ikufotokozanso zimene Mulungu wachita posonyeza kuti amakonda anthu. Nkhani yachiwiri ikufotokoza zimene atumiki a Yehova angachite posonyeza kuti amakonda anzawo.

▪ Zimene Zachitika M’zaka 100 Zimene Ufumu Wakhala Ukulamulira

Nkhaniyi ikufotokoza zimene anthu a Mulungu achita polalikira uthenga wabwino m’zaka 100 zimene Ufumu wakhala ukulamulira. Ikufotokozanso zinthu ndiponso njira zina zimene tagwiritsa ntchito polalikira. M’nkhaniyi tionanso maphunziro amene athandiza kuti abale ndi alongo azilalikira mwaluso.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

13 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

14 Tiziyamikira Zimene Yehova Amatipatsa

31 Kale Lathu

PATSAMBA LOYAMBA: Woyang’anira dera ndiponso apainiya apadera akwera boti kuti apite kumadera a m’nkhalango ya m’mphepete mwa mtsinje wa Amazon. Iwo amasangalala kulalikira uthenga wabwino m’midzi imene ili m’mbali mwa mtsinjewu

BRAZIL

KULI ANTHU

203,067,835

KULI OFALITSA

794,766

KULI APAINIYA

84,550

OPEZEKA PA CHIKUMBUTSO MU 2014

1,728,208

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena