Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w15 12/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 12/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

December 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

FEBRUARY 1-7, 2016

Yehova Amalankhula Nafe

TSAMBA 4

FEBRUARY 8-14, 2016

Baibulo Lomveka Bwino Kwambiri

TSAMBA 9

FEBRUARY 15-21, 2016

Muzigwiritsa Ntchito Bwino Lilime Lanu

TSAMBA 18

FEBRUARY 22-28, 2016

Yehova Adzakuthandizani Pamene Mukudwala

TSAMBA 23

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Yehova Amalankhula Nafe

▪ Baibulo Lomveka Bwino Kwambiri

Kwa zaka zambiri, Yehova wakhala akulankhula ndi atumiki ake m’zilankhulo zosiyanasiyana. M’nkhanizi tikambirana mmene wachitira zimenezi. Tikambirananso mmene Baibulo la Dziko Latsopano lathandizira kuti anthu adziwe dzina la Mulungu ndiponso zimene iye amafuna.

▪ Muzigwiritsa Ntchito Bwino Lilime Lanu

Mulungu anatipatsa mphatso yamtengo wapatali ya kulankhula. M’nkhaniyi tikambirana zinthu zitatu zokhudza kulankhula. Tikambirananso kuti tiyenera kutsanzira Yesu pa nkhani yogwiritsa ntchito mphatsoyi potamanda Mulungu ndiponso kulimbikitsa ena.

▪ Yehova Adzakuthandizani Pamene Mukudwala

Popeza tonsefe timadwala, kodi tingayembekezere kuti Yehova atichiritse mozizwitsa ngati mmene ankachitira ndi anthu ena akale? Kodi tiyenera kuganizira mfundo ziti anthu ena akatipatsa malangizo okhudza mankhwala? Nkhaniyi itithandiza kupeza mayankho a mafunsowa ndiponso kuona mmene tingasankhire zinthu mwanzeru pa nkhani ya mankhwala.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

3 Kodi Mukukumbukira?

14 Baibulo la Dziko Latsopano Lokonzedwanso Lomwe Linatuluka mu 2013

28 Tsopano Ndili pa Mtendere ndi Mulungu Komanso Amayi Anga

32 Mlozera Nkhani wa Magazini a Nsanja ya Olonda a 2015

PATSAMBA LOYAMBA: Mpainiya wapadera akulalikira mayi wina ndiponso ana ake. M’dzikoli anthu ambiri amalankhula Chisipanishi ndi Chiguwarani. Abale ndi alongo amalalikira m’zilankhulo ziwiri zonsezi

PARAGUAY

KULI ANTHU

6,800,236

KULI OFALITSA

9,760

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena