Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w16 April tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
w16 April tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

3 Kodi Utumiki Wanu Uli Ngati Mame?

MLUNGU WA MAY 30, 2016–JUNE 5, 2016

5 Yehova Amadalitsa Anthu Okhulupirika

Nkhaniyi ikufotokoza zimene Yefita ndi mwana wake wamkazi anachita kuti apitirize kutsatira mfundo za Yehova ngakhale kuti ankakumana ndi mavuto. Tiphunziranso kuti kukhala okhulupirika kwa Mulungu n’kofunika kwambiri kuposa chilichonse.

10 Luso Loona Zinthu M’maganizo Mwathu

MLUNGU WA JUNE 6-12, 2016

13 “Mulole Kuti Kupirira Kumalize Kugwira Ntchito Yake”

Tiyenera kupirira mpaka mapeto kuti tidzalandire moyo wosatha. Nkhaniyi ikufotokoza zinthu 4 zimene zingatithandize kupirira komanso zitsanzo za anthu atatu amene anakhalabe okhulupirika pamene ankakumana ndi mavuto. Ikufotokozanso mmene kupirira kungamalizire ntchito yake kwa Mkhristu aliyense.

MLUNGU WA JUNE 13-19, 2016

18 N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kusonkhana?

Akhristufe timakumana ndi mavuto amene angatilepheretse kusonkhana. Nkhaniyi ikufotokoza zimene tingachite kuti tizifikabe pamisonkhano nthawi zonse. Tionanso mmene misonkhano ingatithandizire ifeyo ndi anthu ena komanso mmene Yehova amamvera tikamasonkhana.

23 Mbiri ya Moyo Wanga​—Masisitere Anasintha N’kukhala Alongo

MLUNGU WA JUNE 20-26, 2016

27 Musakhale Mbali ya Dzikoli

Popeza kuti maboma a dzikoli awonongedwa posachedwapa, akhoza kuyamba kutikakamiza kuti tilowerere ndale. Nkhaniyi ikufotokoza zinthu 4 zimene zingatithandize kukhalabe okhulupirika.

32 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena