Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w16 April tsamba 1
  • Magazini Yophunzira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Magazini Yophunzira
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
w16 April tsamba 1
Magazini Yophunzira ya Nsanja ya Olonda ya April 2016

Magazini Yophunzira

April 2016

NKHANI ZOPHUNZIRA KUYAMBIRA: MAY 30 MPAKA JUNE 26, 2016

© 2016 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

PATSAMBA LOYAMBA:

COLOMBIA

Anthu Achiwayu amakonda Mulungu. Abale ndi alongo amayesetsa kuwathandiza kuti amve uthenga wabwino. Anthuwa ali ndi luso loluka zinthu pamanja ndipo amakazigulitsa mumzinda wina wa m’dzikoli. Kumeneko abale amawalalikira uthenga wabwino.

KULI OFALITSA

166,049

MAPHUNZIRO A BAIBULO

229,723

OPEZEKA PA CHIKUMBUTSO (2015)

510,952

Magaziniyi sitigulitsa. Timaipereka ngati njira imodzi yophunzitsira anthu Baibulo padziko lonse ndipo ndalama zoyendetsera ntchitoyi ndi zimene anthu amapereka mwa kufuna kwawo.

Ngati mukufuna kupereka pitani pawebusaiti yathu ya www.pr418.com/ny.

Malemba onse m’magaziniyi akuchokera mu Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika, lolembedwa m’Chichewa chamakono, kupatulapo ngati tasonyeza Baibulo lina.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena