Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w16 July tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
w16 July tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

3 Anadzipereka ndi Mtima Wonse—Ku Ghana

MLUNGU WA AUGUST 29, 2016–SEPTEMBER 4, 2016

7 Muzifunafuna Ufumu Osati Zinthu Zina

Yesu anatiphunzitsa kuti ‘tizifunafuna Ufumu choyamba,’ osati zinthu zina. Kodi tingatani kuti tipewe msampha wokonda chuma komanso kuti tikhale ndi moyo wosalira zambiri n’cholinga choti tiziika zinthu za Ufumu pamalo oyamba? M’nkhaniyi tikambirana mawu a Yesu opezeka pa Mateyu 6:25-34 omwe ananena pa ulaliki wake wapaphiri.

MLUNGU WA SEPTEMBER 5-11, 2016

13 N’chifukwa Chiyani Tiyenera ‘Kukhalabe Maso’?

Masiku otsiriza ano, m’pofunika kwambiri kumvera malangizo a Yesu akuti ‘tikhalebe maso.’ (Mat. 24:42) Kuti zimenezi zitheke, tiyenera kupewa zinthu zimene zingatilepheretse kukhala maso. Nkhaniyi ikufotokoza mmene tingachitire zimenezi.

18 “Usachite Mantha. Ineyo Ndikuthandiza”

MLUNGU WA SEPTEMBER 12-18, 2016

21 Tiziyamikira Kukoma Mtima Kwakukulu kwa Mulungu

MLUNGU WA SEPTEMBER 19-25, 2016

26 Tizilalikira Uthenga wa Kukoma Mtima Kwakukulu kwa Mulungu

Nkhani ziwirizi zikufotokoza mmene kukoma mtima kwakukulu kwa Yehova kumatithandizira. Zikufotokozanso mmene tingasonyezere kuyamikira pothandiza ena kuti nawonso apindule ndi khalidwe la Yehova limeneli.

31 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena