Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w17 October tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
w17 October tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

3 Mbiri ya Moyo Wanga​—Timadalitsidwa Tikamachita Zimene Yehova Amatiuza

MLUNGU WA NOVEMBER 27, 2017–DECEMBER 3, 2017

7 “Tizisonyezana Chikondi Chenicheni M’zochita Zathu”

Akhristu oona amadziwika ndi nkhani yosonyezana chikondi chenicheni. Nkhaniyi ikufotokoza njira 9 zimene tingasonyezere “chikondi chopanda chinyengo.”—2 Akor. 6:6.

MLUNGU WA DECEMBER 4-10, 2017

12 Choonadi Sichibweretsa “Mtendere Koma Lupanga”

Anthu a Yehova amavutika akamatsutsidwa ndi achibale awo omwe si Mboni. Munkhaniyi tiphunzira zimene zingatithandize tikakumana ndi vuto limeneli.

17 Yosefe wa ku Arimateya Analimba Mtima

MLUNGU WA DECEMBER 11-17, 2017

21 Kodi Masomphenya a Zekariya Akukukhudzani Bwanji?

MLUNGU WA DECEMBER 18-24, 2017

26 Timatetezedwa ndi Magaleta Komanso Chisoti Chachifumu

Nkhanizi zikufotokoza masomphenya a nambala 6, 7 ndi 8 amene Zekariya anaona. Masomphenya a nambala 6 ndi 7 atithandiza kuona kuti ndi mwayi waukulu kukhala m’gulu loyera la Mulungu. Masomphenya a nambala 8 akusonyeza mmene Yehova amatitetezera n’cholinga choti tizimulambira moyenera.

31 Anamusonyeza Kukoma Mtima

32 Kodi Mukudziwa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena