Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w18 August tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
w18 August tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

MLUNGU WA OCTOBER 1-7, 2018

3 Kodi Mukudziwa Nkhani Yonse?

MLUNGU WA OCTOBER 8-14, 2018

8 Tisamaweruze Poona Maonekedwe Akunja

Nkhani yoyamba ikufotokoza zinthu zimene zingatilepheretse kudziwa mfundo zonse zokhudza nkhani inayake. Ikufotokozanso mfundo za m’Baibulo zimene zingatithandize kuganizira bwino zimene timadziwa pa nkhani inayake kuti tizindikire zoona zake. Munkhani yachiwiri tikambirana zinthu zitatu zimene zimachititsa munthu kuti aweruze anthu potengera maonekedwe akunja. Ikufotokozanso zimene tingachite kuti tiziweruza anthu mopanda tsankho.

13 Mbiri ya Moyo Wanga​—Ndayesetsa Kuti Ndisagwe Ulesi

MLUNGU WA OCTOBER 15-21, 2018

18 Anthu Opatsa Amakhala Osangalala

MLUNGU WA OCTOBER 22-28, 2018

23 Tizigwira Ntchito ndi Yehova Tsiku Lililonse

Yehova analenga anthu n’cholinga choti akhale ndi moyo wabwino komanso wosangalala. Ngati tsiku lililonse mumachita zinthu zimene zingathandize kuti zolinga za Yehova zikwaniritsidwe ndiye kuti mudzakhala osangalala. Nkhanizi zikufotokozanso ubwino wokhala anthu opatsa m’njira zosiyanasiyana.

28 Kuleza Mtima Ndi Kupirira Kokhala ndi Cholinga

31 Kale Lathu

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena