Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/95 tsamba 7
  • Zilengezo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zilengezo
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—1995
Utumiki Wathu wa Ufumu—1995
km 3/95 tsamba 7

Zilengezo

◼ Mabuku ogwiritsira ntchito mu March: Mafunso Achichepere Akufunsa—Mayankho Amene Amathandiza. April ndi May: Mkupiti wa sabusikripishoni ya Nsanja ya Olonda. June: Baibulo Kodi Ndilo Mawu a Mulungu Kapena a Munthu? CHIDZIŴITSO: Mipingo imene sinaodebe zinthu zamkupiti zotchulidwa pamwambapa iyenera kutero pa fomu yawo ya Literature Request (S-AB-14) yotsatira ya mwezi ndi mwezi.

◼ Woyang’anira wotsogoza kapena wina wosankhidwa ndi iye ayenera kuŵerengera akaunti ya mpingo pa March 1 kapena mwamsanga pambuyo pake. Mutachita zimenezi lengezani ku mpingo.

◼ Nthambi ili ndi timabuku ta Chicheŵa ta “Phunzirani Kuŵerenga ndi Kulemba” m’sitoko. Mipingo ikulimbikitsidwa kuoda timabuku timeneti ndi kuyamba makalasi ophunzira kuŵerenga ndi kulemba.

◼ Kuyambira pa July 3, 1995, brosha lakuti “Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano” ndi buku la Ogwirizana m’Kulambiridwa kwa Mulungu Yekha Wowona, adzaphunziridwa pa Phunziro Labuku Lampingo.

◼ Tikulimbikitsa wofalitsa aliyense kulingalira za kulembetsa upainiya wothandiza m’April.

◼ Zofalitsa Zomwe Zilipo:

Chicheŵa: Kukambitsirana za m’Malemba; Mtendere Weniweni ndi Chisungiko—Kodi Mungazipeze Motani?; Munthu Wamkulu Woposa Onse Amene Anakhalako. Chingelezi: “All Scripture Is Inspired of God and Beneficial”; Chisungiko cha Padziko Lonse mu Ulamuliro wa “Kalonga wa Mtendere”; Mafunso Achichepere Akufunsa—Mayankho Amene Amathandiza; Mankind’s Search for God; mabaundi voliyumu a Watchtower a 1960-93. (Chaka chilichonse chili ndi voliyumu yake ndipo voliyumu imodzi ndi K72.00.) Chonde sonyezani bwino lomwe chaka (zaka) chimene mukufuna pa fomu ya Literature Request (S-AB-14).

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena