Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/96 tsamba 7
  • Kodi Mungayankhe?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mungayankhe?
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—1996
Utumiki Wathu wa Ufumu—1996
km 9/96 tsamba 7

Kodi Mungayankhe?

Kodi munayamba mwaganizapo za mmene mungathetsere vuto la kulankhulana mu ukwati wanu kapena mmene mungathandizire ana anu KUKANA anamgoneka? Kodi mungalithandize bwanji bwenzi limene lili lopsinjika mtima? Kodi mungafotokoze bwino umboni umene tili nawo wakuti Mulungu aliko ndi chimene walolera kuipa? Kodi chilombo chofiiritsa cha m’Chivumbulutso chaputala 17 chimaimiranji? Kapena, kodi nthaŵi zina zimakuvutani kupeza chidziŵitso cha nkhani yanu m’Sukulu Yautumiki Wateokratiki? Tili ndi mavoliyumu ambiri a The Watchtower a zaka zapitazo, 1951-57, 1960-95, ndi Awake! 1984, 85, 87, 1991-95. Chotero kungakhale kothandiza kuwombola mavoliyumu ameneŵa kaamba ka laibulale yanu ngati mulibe. Adzakuthandizani kwambiri pankhani zimenezi. Mtengo wa voliyumu imodzi ndi K72.00 chabe ndipo angaodedwe pakashi kupyolera mumpingo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena