Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/97 tsamba 3
  • Zilengezo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zilengezo
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—1997
Utumiki Wathu wa Ufumu—1997
km 6/97 tsamba 3

Zilengezo

◼ Mabuku ogaŵira mu June: Chidziŵitso Chotsogolera ku Moyo Wosatha. Sumikani maganizo pakuyambitsa maphunziro a Baibulo apanyumba. July ndi August: Lililonse la mabrosha a masamba 32 otsatirawa: Boma Limene Lidzabweretsa Paradaiso, Kodi Chifuno cha Moyo Nchiyani—Kodi Mungachipeze Motani?, Kodi Mulungu Amatisamaliradi?, Kodi Muyenera Kukhulupirira Utatu?, Pamene Munthu Amene Mumakonda Amwalira ndi Sangalalani ndi Moyo Padziko Lapansi Kosatha! September: Chinsinsi cha Chimwemwe cha Banja.

◼ Woyang’anira wotsogoza kapena wina amene iye wamsankha aŵerengere maakaunti a mpingo pa June 1 kapena mwamsanga pambuyo pake. Mutachita zimenezo, lengezani ku mpingo.

◼ Madiski a Nyimbo Omwe Alipo:

Kingdom Melodies 2, 3 (Chonde onani kuti ameneŵa si makaseti iyayi koma madiski ofuna wailesi yapadera. Madiskiwo ali ndi nyimbo zofanana ndi zimene zili pakaseti ndi nambala yomwe).

Singing Kingdom Songs—Chingelezi

◼ Vidiyokaseti Yatsopano Imene Ilipo:

Jehovah’s Witnesses Stand Firm Against Nazi Assault—Chingelezi

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena