Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/09 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 26

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 26
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 26
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 1/09 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa January 26

MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 26

Nyimbo Na. 32

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 13, ndime 9-18

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Genesis 17-20

Na. 1: Genesis 17:1-17

Na. 2: Chifukwa Chake Anthu Alephera Kukhazikitsa Boma Lachilungamo (rs-CN tsa. 62 mpaka tsa. 63 ndime 4)

Na. 3: Mulungu Ali ndi Dzina Lake (lr-CN mutu 4)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 197

Mph. 5: Zilengezo za pampingo.

Mph. 10: Konzekerani Kugawira Magazini ya Nsanja ya Olonda ya February 1 ndi Galamukani! ya February. Kukambirana ndi omvera. Fotokozani mwachidule mfundo za m’magaziniwa ndipo funsani omvera kuti atchule nkhani zimene zingachititse chidwi anthu a m’gawo lanu ndipo anene chifukwa chake. Pemphani omvera kuti atchule zimene anganene poyamba kukambirana ndi munthu. Kodi ndi mafunso komanso malemba ati amene angagwiritse ntchito asanagawire magazini? Malizani nkhaniyi ndi chitsanzo cha mmene tingagawire magazini iliyonse pogwiritsa ntchito mfundo za patsamba 4 kapena mfundo zimene omvera anena.

Mph. 20: “Kodi Mukudziwa Zimene Mungasankhe?”a Nkhani yokambidwa ndi mkulu. Pomaliza, werengani ndime yothera.

Nyimbo Na. 180

[Mawu a M’munsi]

a Mawu anu oyamba asafike mphindi imodzi, ndiyeno kambiranani mwa mafunso ndi mayankho.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena