Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/09 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 2
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 2
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 1/09 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa February 2

MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 2

Nyimbo Na. 136

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 13, ndime 19-23 ndi bokosi

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Genesis 21-24

Na. 1: Genesis 22:1-18

Na. 2: “Uyu Ndiye Mwana Wanga” (lr-CN mutu 5)

Na. 3: Njira Zimene Tingafutukulire Chikondi Chathu pa Ena (2 Akor. 6:11-13)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 220

Mph. 5:  Zilengezo za pampingo. Kumbutsani ofalitsa kuti apereke malipoti awo a utumiki wa kumunda a mwezi wa January.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Mph. 10: Zimene Anthu Amanena Zomwe Zingalepheretse Kukambirana Nawo. Lankhulani mawu oyamba mwachidule, ndipo kenako pogwiritsa ntchito buku la Kukambitsirana, tsamba 15-20, khalani ndi chitsanzo chosonyeza mmene tingayankhire anthu m’gawo lathu ngati anena mawu osonyeza kuti sakufuna kuti tikambirane nawo.

Mph. 10: Thandizani Amene Sakhulupirira Baibulo. Nkhani yokambirana ndi omvera yochokera m’buku la Kukambitsirana, tsamba 58-62. Kambiranani zimene tinganene pa mfundo zosiyanasiyana zimene anthu amanena zotsutsa Baibulo. Khalani ndi chitsanzo chosonyeza mmene tingayankhire mawu amene anthu amakonda kunena m’gawo lathu.

Nyimbo Na. 23

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena