Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/09 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 16

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 16
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 16
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 2/09 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa February 16

MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 16

Nyimbo Na. 98

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 14 ndime 13-20 ndi bokosi

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Genesis 29-31

Na. 1: Genesis 29:1-20

Na. 2: Chifukwa Chake Sitiyenera “Kudera Nkhawa” (Mat. 6: 25)

Na. 3: Kumvera Kumateteza (lr-CN mutu 7)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 172

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 15: “Chitani Zinthu Zonse Kaamba ka Uthenga Wabwino.” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho.

Mph. 15: Kodi Mungachite Upainiya Wothandiza Panyengo ya Chikumbutso? Nkhani yolimbikitsa yokambidwa ndi woyang’anira utumiki. Fotokozani ziyeneretso za apainiya othandiza. Tchulani madalitso amene apainiya othandiza amakhala nawo komanso zimene amasangalala nazo muutumiki. Fotokozani dongosolo lapadera lolowera muutumiki limene mpingo wakonza m’miyezi ya March, April, ndi May. Funsani ofalitsa awiri kapena atatu amene anachita upainiya wothandiza chaka chatha. Kuti athe kuchita upainiya, kodi anasintha chiyani pamoyo wawo? Kodi anapeza madalitso otani? Limbikitsani mabanja kuti akambirane zimene angachite kuti munthu mmodzi kapena angapo m’banjamo achite upainiya wothandiza m’nyengo ya Chikumbutso ikubwerayi.

Nyimbo Na. 151

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena