Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 4/09 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa April 20

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa April 20
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA APRIL 20
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 4/09 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa April 20

MLUNGU WOYAMBIRA APRIL 20

Nyimbo Na. 8

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 18 ndime 1-6

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Eksodo 15-18

Na. 1: Eksodo 15:1-19

Na. 2: Kodi Kupewa Kulambira Konyenga Kumatanthauza Chiyani?

Na. 3: Phunziro la Kukhala Wokoma Mtima (lr-CN mutu 15)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 49

Mph.5: Zilengezo.

Mph.15: Konzekerani kugawira magazini ya Nsanja ya Olonda ya May 1 ndi Galamukani! ya May. Funsani omvera kuti atchule nkhani zimene zingachititse chidwi anthu a m’gawo lanu ndipo anene chifukwa chake. Chitani chitsanzo cha mmene mungagawire magazini iliyonse. Mu chitsanzo chimodzi, sonyezani mmene mungayambitsire phunziro pa ulendo wobwereza.—Onani Utumiki Wathu wa Ufumu wa August 2007, tsamba 3.

Mph.15: “Phunzitsani Anthu Amene Amavutika Kuwerenga.” Pokambirana ndime 3, chitani chitsanzo chachidule chosonyeza mpainiya akugwiritsa ntchito bwino chithunzi chimene chili m’buku limene akuphunzitsira.

Nyimbo Na. 170

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena