Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/09 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 17

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 17
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 17
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 8/09 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa August 17

MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 17

Nyimbo Na. 225

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 24, ndime 1-10

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Numeri 10-13

Na. 1: Numeri 13:17-33

Na. 2: Zimene Zingatithandize Kuthetsa Mantha (lr-CN mutu 30)

Na. 3: Kodi Lemba la 1 Petulo 3:19, 20 Limatanthauza Chiyani? (rs-CN tsa. 205, ndime 2)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 36

Mph.5: Zilengezo.

Mph.15: Kulalikira Nyumba ndi Nyumba. Nkhani yokambirana ndi omvetsera kuchokera m’buku la Gulu, tsamba 92, ndime 3 mpaka tsamba 95, ndime 2. Funsani wofalitsa mmodzi kapena awiri amene amalalikira ku nyumba ndi nyumba ngakhale kuti ali ndi mavuto amene angawalepheretse kutero, monga kudwaladwala kapena manyazi. Kodi apeza madalitso otani chifukwa cha khama lawo?

Mph.15: “Kodi Mwakonzekera Kukalalikira Kusukulu?” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho. Funsani wachinyamata mmodzi kapena awiri amene analalikirapo kusukulu. Kodi chinawathandiza n’chiyani? Apempheni kuti afotokoze mmene zinachitikira.

Nyimbo Na. 221

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena