Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/09 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 16

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 16
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 16
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 11/09 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa November 16

MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 16

Nyimbo Na. 62

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 29 ndime 13-21, ndi bokosi patsamba 299

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Deuteronomo 23-27

Na. 1: Deuteronomo 25:1-16

Na. 2: Ana Amene Amakondweretsa Mulungu (lr-CN mutu 41)

Na. 3: Kodi Ndi Zinthu Ziti Zimene Tiyenera Kuziona Kukhala Zopatulika?

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 146

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Khalani Wozindikira Ndipo Afikeni Pamtima Anthu. Nkhani yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 258, ndime 1, mpaka tsamba 259, ndime 3.

Mph. 10: Tsogolerani Anthu Achidwi ku Gulu la Yehova. Nkhani yokambirana ndi omvera kuchokera m’buku la Gulu, patsamba 99, ndime 2, mpaka patsamba 100, ndime 1. Chitaninso chitsanzo chachidule chosonyeza mfundo imodzi pa mfundo zimene zafotokozedwa m’nkhaniyi.

Mph. 10: “Yakani ndi Mzimu.” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 16

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena