Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/10 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 15

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 15
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 15
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 2/10 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa February 15

MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 15

Nyimbo Na. 54

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 3 ndime 16-21

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Oweruza 15-18

Na. 1: Oweruza 16:1-12

Na. 2: Kodi ‘Gehena wa Moto’ Amene Yesu Anatchula Ndi Chiyani? (rs tsa.148 ndime 1–tsa.149 ndime 1)

Na. 3: N’chifukwa Chiyani Yesu Anatcha Mdyerekezi “Tate Wake wa Bodza”? (Yoh. 8:44)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 13

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 15: Konzekerani Kugawira Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! Kambiranani mwachidule nkhani za m’magaziniwa ndipo tchulani nkhani zimene anthu a m’gawo lanu angasangalale nazo. Sonyezani wofalitsa akulankhula yekhayekha pokonzekera kugawira magaziniwa. Iye asankhe nkhani zimene akuona kuti anthu a m’gawo lanu angachite nazo chidwi kwambiri. Ndiyeno akonze funso ndiponso asankhe malemba amene angagwiritse ntchito. Pomaliza, iye ayerekezere kugawira magazini iliyonse payokha.

Mph. 15: “Msonkhano Wadera Umene Udzatithandize Kuteteza Moyo Wathu Wauzimu.” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 21

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena