Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/10 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 24

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 24
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MAY 24
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 5/10 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa May 24

MLUNGU WOYAMBIRA MAY 24

Nyimbo Na. 37

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 7 ndime 10-19 ndi bokosi patsamba 81

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Samueli 13-15

Na. 1: 2 Samueli 13:23-33

Na. 2: Kodi Tiyenera Kugwiritsa Ntchito Zifaniziro Polambira Mulungu Woona? (rs tsa. 435 ndime 4 mpaka ndime 8)

Na. 3: N’chifukwa Chiyani Sitiyenera Kugwiritsa Ntchito Dzikoli Mokwanira, Kapena Kuti Mopitirira Malire? (1 Akor. 7:31)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 32

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Konzekerani Kudzagawira magazini mu June. Nkhani yokambirana ndi omvetsera. Fotokozani zimene zili m’magaziniwo kwa mphindi imodzi kapena ziwiri. Kenako sankhani nkhani zina, ndipo pemphani omvetsera kuti anene mafunso ndiponso malemba amene angagwiritsire ntchito pogawira magaziniwo. Chitani chitsanzo chosonyeza zimene tingachite pogawira magazini iliyonse.

Mph. 20: “Upainiya Ungakuyenereni Kwabasi!” Nkhani ya mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 26

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena