Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/10 tsamba 8
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 7

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 7
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 7
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 5/10 tsamba 8

Ndandanda ya Mlungu wa June 7

MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 7

Nyimbo Na. 48

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv Zakumapeto kuyambira pakamutu patsamba 215-218

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Samueli 19-21

Na. 1: 2 Samueli 19:11-23

Na. 2: Kodi Mulungu Amaona Bwanji Zifaniziro Zimene Anthu Amagwiritsa Ntchito Polambira? (rs tsa. 437 ndime 1-4)

Na. 3: Njira Zimene Mdyerekezi Amachititsira Anthu Khungu Kuti Asadziwe Choonadi (2 Akor. 4:4)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 23

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Lalikirani Zomveka Bwino kwa Ena. Nkhani yokambirana ndi omvera yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 226-229.

Mph. 10: Zosowa za Pampingo.

Mph. 10: Njira Zolalikirira Uthenga Wabwino—Kugwira Ntchito M’magawo Omwe Anthu Amalankhula Zinenero Zosiyanasiyana. Nkhani yokambirana ndi omvera yochokera m’buku la Gulu, tsamba 107, ndime 1 ndi 2. Mwachidule, funsani woyang’anira utumiki kuti atchule mipingo ya zinenero zina imene imalalikiranso m’gawo lanu. Kodi pali dongosolo lotani limene mipingoyo inagwirizana pofuna kuti aliyense m’gawolo alalikiridwe komanso kuti munthu mmodzi asamalalikiridwe ndi anthu awiri a zinenero zosiyana?

Nyimbo Na. 28

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena